Job 25 – NVI & CCL

Nueva Versión Internacional

Job 25:1-6

Tercer discurso de Bildad

1A esto respondió Bildad de Súah:

2«Dios es poderoso e infunde temor;

él pone orden en las alturas de los cielos.

3¿Pueden contarse acaso sus ejércitos?

¿Sobre quién no alumbra su luz?

4¿Cómo puede una persona declararse justo ante Dios?

¿Cómo puede alegar pureza quien ha nacido de mujer?

5Si a sus ojos no tiene brillo la luna,

ni son puras las estrellas,

6mucho menos el hombre, simple gusano;

¡mucho menos el hombre, miserable lombriz!».

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 25:1-6

Mawu a Bilidadi

1Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,

Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.

3Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?

Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?

4Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?

Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?

5Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,

ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,

6nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,

mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”