Psalm 114 – NIRV & CCL

New International Reader’s Version

Psalm 114:1-8

Psalm 114

1The people of Israel came out of Egypt.

The people of Jacob left a land where a different language was spoken.

2Then Judah became the holy place where God lived.

Israel became the land he ruled over.

3The Red Sea saw him and parted.

The Jordan River stopped flowing.

4The mountains leaped like rams.

The hills skipped like lambs.

5Red Sea, why did you part?

Jordan River, why did you stop flowing?

6Why did you mountains leap like rams?

Why did you hills skip like lambs?

7Earth, tremble with fear when the Lord comes.

Tremble when the God of Jacob is near.

8He turned the rock into a pool.

He turned the hard rock into springs of water.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 114:1-8

Salimo 114

1Pamene Israeli anatuluka mu Igupto,

nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,

2Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu,

Israeli anasanduka ufumu wake.

3Nyanja inaona ndi kuthawa,

mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;

4mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna,

timapiri ngati ana ankhosa.

5Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa?

iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?

6inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna,

inu timapiri, ngati ana ankhosa?

7Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi,

pamaso pa Mulungu wa Yakobo,

8amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime,

thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.