Zaburi 67 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 67:1-7

Zaburi 67

Mataifa Yahimizwa Kumsifu Mungu

Kwa mwimbishaji. Na ala za nyuzi za muziki. Zaburi. Wimbo.

167:1 Hes 6:24-26; Za 4:6; 31:16; 119:135; 2Kor 4:6Mungu aturehemu na kutubariki,

na kutuangazia nuru za uso wake,

267:2 Isa 40:5; 52:10; 62:1, 2; Lk 2:30-32; Tit 2:11; Za 98:2; Mdo 10:35; 13:10ili njia zako zijulikane duniani,

wokovu wako katikati ya mataifa yote.

367:3 Za 67:5; Isa 24:15, 16Ee Mungu, mataifa na wakusifu,

mataifa yote na wakusifu.

467:4 Za 100:1-2; 9:4; 96:10-13; 68:32Mataifa yote wafurahi na kuimba kwa shangwe,

kwa kuwa unatawala watu kwa haki

na kuongoza mataifa ya dunia.

567:5 Za 67:3Ee Mungu, mataifa na wakusifu,

mataifa yote na wakusifu.

667:6 Mwa 8:22; 12:2; Law 26:4; Za 85:12; Isa 55:10; Eze 34:27; Zek 8:12Ndipo nchi itatoa mazao yake,

naye Mungu, Mungu wetu, atatubariki.

767:7 Za 2:8; 33:8Mungu atatubariki

na miisho yote ya dunia itamcha yeye.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.