Zaburi 48 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 48:1-14

Zaburi 48

Sayuni, Mji Wa Mungu

Wimbo. Zaburi ya wana wa Kora.

148:1 2Sam 22:4; Mik 4:1; Yer 10:6; 31:23; Za 86:10; 96:4; 99:2; 135:5; 147:5; 46:4; 87:1; 18:3; 2:6; 1Nya 16:25; Kum 33:19; Isa 2:2; 11:9; 32:16; Zek 8:3; Oba 1:17; Dan 9:16Bwana ni mkuu, anayestahili kusifiwa sana,

katika mji wa Mungu wetu,

mlima wake mtakatifu.

248:2 Isa 14:13; Za 2:6; 50:2; Mao 2:15; Eze 16:14; 20:6; Yos 13:17; Mt 5:35; Yer 3:19Ni mzuri katika kuinuka kwake juu sana,

furaha ya dunia yote.

Kama vilele vya juu sana vya Safoni48:2 Safoni inaweza ikawa na maana ya mlima mtakatifu au upande wa kaskazini. ni Mlima Sayuni,

mji wa Mfalme Mkuu.

348:3 Za 122:7; 18:2Mungu yuko katika ngome zake;

amejionyesha mwenyewe kuwa ngome yake.

448:4 2Sam 10:1-19Wakati wafalme walipounganisha nguvu,

waliposonga mbele pamoja,

548:5 Kut 15:16walimwona nao wakashangaa,

wakakimbia kwa hofu.

648:6 Ay 4:14; Mwa 3:16Kutetemeka kuliwashika huko,

maumivu kama ya mwanamke

mwenye utungu wa kuzaa.

748:7 Mwa 10:4; 41:6; 1Fal 10:22; 22:48; Eze 27:26Uliwaangamiza kama meli za Tarshishi

zilizovunjwa na upepo wa mashariki.

848:8 Yer 23:6; Mik 4:1; Zek 8:13; 14:11; Isa 2:2Kama tulivyokuwa tumesikia,

ndivyo tulivyoona

katika mji wa Bwana Mwenye Nguvu Zote,

katika mji wa Mungu wetu:

Mungu ataufanya uwe salama milele.

948:9 Za 39:3; 6:4Ee Mungu, hekaluni mwako

tunatafakari upendo wako usiokoma.

1048:10 Kut 6:3; Isa 11:12; 24:16; 42:10; 49:6; Yos 7:9; 1Sam 2:10; Za 22:27; 100:1; 65:5; 98:3; Mal 1:1Ee Mungu, kama jina lako lilivyo,

sifa zako zinafika hadi miisho ya dunia,

mkono wako wa kuume umejazwa na haki.

1148:11 Za 97:8Mlima Sayuni unashangilia,

vijiji vya Yuda vinafurahi

kwa sababu ya hukumu zako.

1248:12 Neh 3:1Tembeeni katika Sayuni,

uzungukeni mji,

hesabuni minara yake;

1348:13 2Sam 20:15; Isa 26:1; Mao 2:8; Hab 2:1; Za 78:6; 71:18; 109:13yatafakarini vyema maboma yake,

angalieni ngome zake,

ili mpate kusimulia habari zake

kwa kizazi kijacho.

1448:14 Za 25:5; 73:24; Mit 6:22; Isa 25:9; 49:10; 57:18; 58:11Kwa kuwa huyu Mungu ni Mungu wetu milele na milele;

atakuwa kiongozi wetu hata mwisho.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 48:1-14

Salimo 48

Nyimbo. Salimo la ana a Kora.

1Wamkulu ndi Yehova, ndi woyenera kwambiri matamando

mu mzinda wa Mulungu wathu, phiri lake loyera.

2Lokongola mu utali mwake,

chimwemwe cha dziko lonse lapansi.

Malo aatali kwambiri a Zafoni ndiye Phiri la Ziyoni,

mzinda wa Mfumu yayikulu.

3Mulungu ali mu malinga ake;

Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.

4Pamene mafumu anasonkhana pamodzi,

pamene anayendera pamodzi kudzalimbana nafe,

5iwo anaona mzindawo ndipo anadabwa kwambiri;

anathawa ndi mantha aakulu.

6Pomwepo anagwidwa nako kunjenjemera,

ululu wonga wa mkazi woyembekezera pa nthawi yochira.

7Inu munawawononga monga sitima zapamadzi za ku Tarisisi

zitawonongeka ndi mphepo ya kummawa.

8Monga momwe tinamvera,

kotero ife tinaona

mu mzinda wa Yehova Wamphamvuzonse,

mu mzinda wa Mulungu wathu.

Mulungu adzawuteteza kwamuyaya.

9Mʼkati mwa Nyumba yanu Mulungu,

ife timalingaliramo zachikondi chanu chosasinthika.

10Monga dzina lanu, Inu Mulungu,

matamando anu amafika ku malekezero a dziko lapansi

dzanja lanu lamanja ladzaza ndi chilungamo.

11Phiri la Ziyoni likukondwera,

midzi ya Yuda ndi yosangalala

chifukwa cha maweruzo anu.

12Yendayendani mu Ziyoni, uzungulireni mzindawo,

werengani nsanja zake.

13Yangʼanitsitsani bwino mipanda yake,

penyetsetsani malinga ake,

kuti mudzafotokoze za izo ku mʼbado wotsatira.

14Pakuti Mulungu uyu ndi Mulungu wathu ku nthawi zosatha;

Iye adzakhala mtsogoleri wathu mpaka ku mapeto.