Zaburi 32 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 32:1-11

Zaburi 32

Furaha Ya Msamaha

Zaburi ya Daudi. Funzo.

132:1 Za 85:2; 103:3; Rum 4:6Heri mtu yule ambaye amesamehewa makosa yake,

ambaye dhambi zake zimefunikwa.

232:2 Rum 4:7-8; 5:13; Yn 1:47; Ufu 14:5; 2Kor 1:12; Law 17:4Heri mtu yule ambaye Bwana

hamhesabii dhambi,

na ambaye rohoni mwake

hamna udanganyifu.

332:3 Ay 31:34; 31:10; 3:24; Za 6:6Niliponyamaza, mifupa yangu ilichakaa

kwa kulia kwa maumivu makali mchana kutwa.

432:4 1Sam 5:6; Ay 9:34; Za 38:2; 39:10; 22:15Usiku na mchana

mkono wako ulinilemea,

nguvu zangu zilinyonywa

kama vile katika joto la kiangazi.

532:5 Ay 31:33; Mit 28:13; Lk 15:18; Za 103:12; Law 26:40; Yn 1:9Kisha nilikujulisha dhambi yangu

wala sikuficha uovu wangu.

Nilisema, “Nitaungama

makosa yangu kwa Bwana.”

Ndipo uliponisamehe

hatia ya dhambi yangu.

632:6 Za 69:13; Yn 7:34; Isa 55:6; Za 69:1; 43:2; Kut 15:10; 1Tim 1:16Kwa hiyo kila mtu mcha Mungu akuombe

wakati unapopatikana,

hakika maji makuu yatakapofurika

hayatamfikia yeye.

732:7 Za 9:9; Amu 9:35; 5:1; Mit 18:10; Isa 4:6; Mt 23:37; Kol 3:3Wewe ndiwe mahali pangu pa kujificha,

utaniepusha na taabu

na kunizunguka kwa nyimbo za wokovu.

832:8 Za 25:8; 34:11; 33:18; Isa 48:17Nitakufundisha na kukuonyesha njia utakayoiendea;

nitakushauri na kukuangalia.

932:9 Ay 30:11; 39:10; Yak 3:3Usiwe kama farasi au nyumbu

wasio na akili,

ambao ni lazima waongozwe kwa lijamu na hatamu

la sivyo hawatakukaribia.

1032:10 Rum 2:9; Za 4:5; Mit 16:20; Yer 17:7; Mit 13:21; 16:20Mtu mwovu ana taabu nyingi,

bali upendo usio na kikomo wa Bwana

unamzunguka mtu anayemtumaini.

1132:11 Za 64:10Shangilieni katika Bwana na mfurahi, enyi wenye haki!

Imbeni, nyote mlio wanyofu wa moyo!

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 32:1-11

Salimo 32

Salimo la Davide. Malangizo.

1Ngodala munthu

amene zolakwa zake zakhululukidwa;

amene machimo ake aphimbidwa.

2Ngodala munthu

amene machimo ake Yehova sawawerengeranso pa iye

ndipo mu mzimu mwake mulibe chinyengo.

3Pamene ndinali chete,

mafupa anga anakalamba

chifukwa cha kubuwula kwanga tsiku lonse.

4Pakuti usana ndi usiku

dzanja lanu linandipsinja;

mphamvu zanga zinatha

monga nthawi yotentha yachilimwe.

Sela

5Kotero ine ndinavomereza tchimo langa kwa Inu,

sindinabise mphulupulu zanga.

Ndinati, “Ine ndidzawulula

zolakwa zanga kwa Yehova,

ndipo Inu munandikhululukira

mlandu wa machimo anga.”

Sela

6Choncho aliyense okhulupirika apemphere kwa Inuyo

pomwe mukupezeka;

ndithu pamene madzi amphamvu auka,

sadzamupeza.

7Inu ndi malo anga obisala;

muzinditeteza ku mavuto ndipo muzindizinga

ndi nyimbo zachipulumutso.

Sela

8Ndidzakulangiza ndi kukuphunzitsa njira imene udzayendamo;

ndidzakupatsa uphungu ndi kukuyangʼanira.

9Usakhale ngati kavalo kapena bulu,

zimene zilibe nzeru,

koma ziyenera kuwongoleredwa ndi zitsulo za mʼkamwa ndi pamutu,

ukapanda kutero sizibwera kwa iwe.

10Zowawa ndi zambiri za anthu oyipa

koma chikondi chosatha cha Yehova

chimamuzinga munthu amene amadalira Iye.

11Kondwerani mwa Yehova inu olungama;

imbani, inu nonse amene muli owongoka mtima!