Zaburi 136 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 136:1-26

Zaburi 136

Wimbo Wa Kumshukuru Mungu

1136:1 Za 105:1; 100:5; 145:9; 118:1-4; 106:1; Ezr 3:11; Hes 2:26; 1:7; 2Nya 5:13; Yer 33:11Mshukuruni Bwana, kwa kuwa ni mwema.

Fadhili zake zadumu milele.

2136:2 Za 105:1; Kum 10:17; Kut 18:11Mshukuruni Mungu wa miungu.

Fadhili zake zadumu milele.

3136:3 Za 105:1; Kum 10:17; 1Tim 6:15Mshukuruni Bwana wa mabwana:

Fadhili zake zadumu milele.

4136:4 Kut 3:20; Ay 9:10Kwake yeye pekee atendaye maajabu makuu,

Fadhili zake zadumu milele.

5136:5 Mit 3:19; Yer 51:15; Mwa 1:1Ambaye kwa ufahamu wake aliziumba mbingu,

Fadhili zake zadumu milele.

6136:6 Mwa 1:1; 1:6; Isa 42:5; Yer 10:12; 33:2Ambaye aliitandaza dunia juu ya maji,

Fadhili zake zadumu milele.

7136:7 Mwa 1:14, 16; Za 74:16; Yak 1:17Ambaye aliumba mianga mikubwa,

Fadhili zake zadumu milele.

8136:8 Mwa 1:16Jua litawale mchana,

Fadhili zake zadumu milele.

9Mwezi na nyota vitawale usiku,

Fadhili zake zadumu milele.

10136:10 Kut 4:23; 12:12Kwake yeye aliyemuua mzaliwa wa kwanza wa Misri,

Fadhili zake zadumu milele.

11136:11 Kut 6:6; 13:3; Za 105:43Na kuwatoa Israeli katikati yao,

Fadhili zake zadumu milele.

12136:12 Kut 3:20; Kum 5:15; 9:29Kwa mkono wenye nguvu ulionyooshwa,

Fadhili zake zadumu milele.

13136:13 Za 78:13Kwake yeye aliyeigawa Bahari ya Shamu,

Fadhili zake zadumu milele.

14136:14 Kut 14:22; Za 106:9Na kuwapitisha Israeli katikati yake,

Fadhili zake zadumu milele.

15136:15 Kut 14:27Lakini alimfagia Farao na jeshi lake katika Bahari ya Shamu,

Fadhili zake zadumu milele.

16136:16 Kut 13:18; Za 78:52Kwake yeye aliyewaongoza watu wake katika jangwa,

Fadhili zake zadumu milele.

17136:17 Hes 21:23-25; Yos 24:8-11; Za 78:55; 135:9-12Ambaye aliwapiga wafalme wenye nguvu,

Fadhili zake zadumu milele.

18136:18 Kum 29:7; Yos 12:7-24Naye aliwaua wafalme wenye nguvu,

Fadhili zake zadumu milele.

19136:19 Hes 21:21-25Sihoni mfalme wa Waamori,

Fadhili zake zadumu milele.

20136:20 Hes 21:33-35Ogu mfalme wa Bashani,

Fadhili zake zadumu milele.

21136:21 Kum 1:38; Yos 12:1; 14:1Akatoa nchi yao kuwa urithi,

Fadhili zake zadumu milele.

22136:22 Kum 29:8; Za 78:55; Isa 20:3; 41:8; 42:19; 43:10; 44:1, 21; 45:4; 49:5-7Urithi kwa Israeli mtumishi wake,

Fadhili zake zadumu milele.

23136:23 Za 78:29; 103:14; 115:12Aliyetukumbuka katika unyonge wetu,

Fadhili zake zadumu milele.

24136:24 Yos 10:14; Neh 9:28; Kum 6:19Alituweka huru toka adui zetu,

Fadhili zake zadumu milele.

25136:25 Mwa 1:30; Mit 6:26Ambaye humpa chakula kila kiumbe.

Fadhili zake zadumu milele.

26136:26 Za 105:1; 115:3; Ezr 3:11Mshukuruni Mungu wa mbinguni,

Fadhili zake zadumu milele.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 136:1-26

Salimo 136

1Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.

Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

2Yamikani Mulungu wa milungu.

Pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

3Yamikani Ambuye wa ambuye,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

4Iye yekhayo amene amachita zodabwitsa zazikulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

5Amene mwachidziwitso chake anapanga mayiko akumwamba,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

6Amene anayala dziko lapansi pamwamba pa madzi,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

7Amene anapanga miyuni ikuluikulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

8Dzuwa lilamulire usana,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

9Mwezi ndi nyenyezi zilamulire usiku,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

10Amene anakantha ana woyamba kubadwa a Igupto,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

11Natulutsa Israeli pakati pawo,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

12Ndi dzanja lamphamvu ndi mkono wotambasuka,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

13Amene anagawa Nyanja Yofiira pakati,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

14Nadutsitsa Israeli pakati pa nyanjayo,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

15Koma anakokolola Farao ndi ankhondo ake mʼNyanja Yofiira,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

16Amene anatsogolera anthu ake mʼchipululu

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

17Amene anakantha mafumu akuluakulu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

18Napha mafumu amphamvu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

19Siloni mfumu ya Aamori,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

20Ogi mfumu ya Basani,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

21Napereka dziko lawo ngati cholowa,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

22Cholowa cha mtumiki wake Israeli;

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

23Amene anatikumbukira ife anthu opeputsidwa,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

24Amene anatimasula kwa adani athu,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

25Amene amapereka chakudya kwa cholengedwa chilichonse,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.

26Yamikani Mulungu wakumwamba,

pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya.