Zaburi 13 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 13:1-6

Zaburi 13

Sala Ya Kuomba Msaada

Kwa mwimbishaji. Zaburi ya Daudi.

113:1 Mao 5:20; Kum 31:17; Za 6:3; 22:1, 14; 42:9; Isa 8:17; 54:9; 59:2; Ay 13:2413:1 Kum 26:7; 32:20Mpaka lini, Ee Bwana? Je, utanisahau milele?

Utanificha uso wako mpaka lini?

213:2 Za 42:4; 55:2; 94:3; 139:23; Isa 33:18; Dan 7:28Nitapambana na mawazo yangu mpaka lini,

na kila siku kuwa na majonzi moyoni mwangu?

Adui zangu watanishinda mpaka lini?

313:3 Za 4:1; 9:12; 31:7; 18:28; 25:18; 35:23; 59:4; 80:14; 107:41; 119:50, 53; Lk 2:32; Efe 5:14; Ufu 21:23; Isa 37:36Nitazame, unijibu, Ee Bwana Mungu wangu.

Yatie nuru macho yangu,

ama sivyo nitalala usingizi wa mauti.

413:4 1Fal 19:2; Za 25:2; 38:16; 118:13Adui yangu atasema, “Nimemshinda,”

nao adui zangu watashangilia nitakapoanguka.

513:5 Ay 33:26; Isa 25:9; 33:2; Za 6:4; 9:14; 2Nya 20:12Lakini ninategemea upendo wako usiokoma;

moyo wangu unashangilia katika wokovu wako.

613:6 Kut 15:1; Za 7:17Nitamwimbia Bwana,

kwa kuwa amekuwa mwema kwangu.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 13:1-6

Salimo 13

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide.

1Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale?

Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?

2Ndidzalimbana ndi maganizo anga

ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti?

Mpaka liti adani anga adzandipambana?

3Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga.

Walitsani maso anga kuti ndingafe;

4mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,”

ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.

5Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika;

mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.

6Ine ndidzayimbira Yehova

pakuti wandichitira zokoma.