Zaburi 127 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 127:1-5

Zaburi 127

Bila Mungu, Kazi Ya Mwanadamu Haifai

Wimbo wa kwenda juu. Wa Solomoni.

1127:1 Za 78:69; 121:4Bwana asipoijenga nyumba,

wajengao hufanya kazi bure.

Bwana asipoulinda mji,

walinzi wakesha bure.

2127:2 Mwa 3:17; Hes 6:26; Ay 11:18; Kum 33:12; Mhu 2:25Mnajisumbua bure kuamka mapema

na kuchelewa kulala,

mkitaabikia chakula:

kwa maana yeye huwapa usingizi wapenzi wake.

3127:3 Mwa 1:28; 33:5; Kum 28:4Wana ni urithi utokao kwa Bwana,

watoto ni zawadi kutoka kwake.

4127:4 Za 112:2Kama mishale mikononi mwa shujaa

ndivyo walivyo wana awazaao mtu katika ujana wake.

5127:5 Za 128:2-3; Mwa 24:60; 23:10Heri mtu ambaye podo lake

limejazwa nao.

Hawataaibishwa wanaposhindana

na adui zao langoni.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 127:1-5

Salimo 127

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni.

1Yehova akapanda kumanga nyumba,

omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe.

Yehova akapanda kulondera mzinda,

mlonda akanangolondera pachabe.

2Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa

ndi kusagona msanga madzulo,

kuvutikira chakudya choti mudye,

pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.

3Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,

ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.

4Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja

mwa munthu wankhondo.

5Wodala munthu

amene motengera mivi mwake mwadzaza.

Iwo sadzachititsidwa manyazi

pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.