Zaburi 127
Bila Mungu, Kazi Ya Mwanadamu Haifai
Wimbo wa kwenda juu. Wa Solomoni.
1127:1 Za 78:69; 121:4Bwana asipoijenga nyumba,
wajengao hufanya kazi bure.
Bwana asipoulinda mji,
walinzi wakesha bure.
2127:2 Mwa 3:17; Hes 6:26; Ay 11:18; Kum 33:12; Mhu 2:25Mnajisumbua bure kuamka mapema
na kuchelewa kulala,
mkitaabikia chakula:
kwa maana yeye huwapa usingizi wapenzi wake.
3127:3 Mwa 1:28; 33:5; Kum 28:4Wana ni urithi utokao kwa Bwana,
watoto ni zawadi kutoka kwake.
4127:4 Za 112:2Kama mishale mikononi mwa shujaa
ndivyo walivyo wana awazaao mtu katika ujana wake.
5127:5 Za 128:2-3; Mwa 24:60; 23:10Heri mtu ambaye podo lake
limejazwa nao.
Hawataaibishwa wanaposhindana
na adui zao langoni.
Salimo 127
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni.
1Yehova akapanda kumanga nyumba,
omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe.
Yehova akapanda kulondera mzinda,
mlonda akanangolondera pachabe.
2Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa
ndi kusagona msanga madzulo,
kuvutikira chakudya choti mudye,
pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.
3Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova,
ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
4Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja
mwa munthu wankhondo.
5Wodala munthu
amene motengera mivi mwake mwadzaza.
Iwo sadzachititsidwa manyazi
pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.