Zaburi 12
Kuomba Msaada
Kwa mwimbishaji. Mtindo wa sheminithi. Zaburi ya Daudi.
112:1 Isa 57:1; Mik 7:12Bwana tusaidie, kwa kuwa wacha Mungu wametoweka;
waaminifu wametoweka miongoni mwa wanadamu.
212:2 Za 5:6; 34:13; 141:3; 5:9; Mt 6:19; 12:17; 13:3; Isa 32:7; Rum 16:18Kila mmoja humwambia jirani yake uongo;
midomo yao ya hila huzungumza kwa udanganyifu.
312:3 Mit 26:28; 28:23; Za 73:9; Ufu 13:5; Dan 7:8; Yak 3:5Bwana na akatilie mbali midomo yote ya hila
na kila ulimi uliojaa majivuno,
412:4 Mt 18:21; Yak 3:6ule unaosema, “Kwa ndimi zetu tutashinda;
midomo ni mali yetu, bwana wetu ni nani?”
512:5 Kut 3:7, 8; Mhu 4:1, 5, 8; Isa 3:15; 5:7; 30:12; 59:13; Mdo 7:34; Za 44:24; 62:10; 72:14; 73:8; 6:6; 3:7; 34:6; 35:10“Kwa sababu ya uonevu wa wanyonge
na kulia kwa uchungu kwa wahitaji,
nitainuka sasa,” asema Bwana.
“Nitawalinda kutokana na wale
wenye nia mbaya juu yao.”
612:6 2Sam 22:31; Isa 48:10; Za 18:30; 119:140; Ay 23:10; 28:1; Zek 13:9Maneno ya Bwana ni safi,
kama fedha iliyosafishwa katika tanuru,
iliyosafishwa mara saba.
712:7 Za 16:1; 27:5; 37:28; Yn 17:12Ee Bwana, utatuweka salama
na kutulinda na kizazi hiki milele.
812:8 Za 55:10-11Watu waovu huenda wakiringa kila mahali
wakati ambapo yule aliye mbaya sana
ndiye anayeheshimiwa miongoni mwa watu.
Salimo 12
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide.
1Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;
okhulupirika akusowa pakati pa anthu.
2Aliyense amanamiza mʼbale wake;
ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.
3Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo
ndi pakamwa paliponse podzikuza.
4Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;
pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”
5“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu
ndi kubuwula kwa anthu osowa,
Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova,
“Ndidzawateteza kwa owazunza.”
6Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro
monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi,
oyengedwa kasanu nʼkawiri.
7Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo
mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.
8Oyipa amangoyendayenda ponseponse
anthu akamayamikira zochita zawo.