Zaburi 12 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 12:1-8

Zaburi 12

Kuomba Msaada

Kwa mwimbishaji. Mtindo wa sheminithi. Zaburi ya Daudi.

112:1 Isa 57:1; Mik 7:12Bwana tusaidie, kwa kuwa wacha Mungu wametoweka;

waaminifu wametoweka miongoni mwa wanadamu.

212:2 Za 5:6; 34:13; 141:3; 5:9; Mt 6:19; 12:17; 13:3; Isa 32:7; Rum 16:18Kila mmoja humwambia jirani yake uongo;

midomo yao ya hila huzungumza kwa udanganyifu.

312:3 Mit 26:28; 28:23; Za 73:9; Ufu 13:5; Dan 7:8; Yak 3:5Bwana na akatilie mbali midomo yote ya hila

na kila ulimi uliojaa majivuno,

412:4 Mt 18:21; Yak 3:6ule unaosema, “Kwa ndimi zetu tutashinda;

midomo ni mali yetu, bwana wetu ni nani?”

512:5 Kut 3:7, 8; Mhu 4:1, 5, 8; Isa 3:15; 5:7; 30:12; 59:13; Mdo 7:34; Za 44:24; 62:10; 72:14; 73:8; 6:6; 3:7; 34:6; 35:10“Kwa sababu ya uonevu wa wanyonge

na kulia kwa uchungu kwa wahitaji,

nitainuka sasa,” asema Bwana.

“Nitawalinda kutokana na wale

wenye nia mbaya juu yao.”

612:6 2Sam 22:31; Isa 48:10; Za 18:30; 119:140; Ay 23:10; 28:1; Zek 13:9Maneno ya Bwana ni safi,

kama fedha iliyosafishwa katika tanuru,

iliyosafishwa mara saba.

712:7 Za 16:1; 27:5; 37:28; Yn 17:12Ee Bwana, utatuweka salama

na kutulinda na kizazi hiki milele.

812:8 Za 55:10-11Watu waovu huenda wakiringa kila mahali

wakati ambapo yule aliye mbaya sana

ndiye anayeheshimiwa miongoni mwa watu.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 12:1-8

Salimo 12

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Monga mwa mayimbidwe seminiti. Salimo la Davide.

1Thandizeni Yehova pakuti palibe munthu wokhulupirika;

okhulupirika akusowa pakati pa anthu.

2Aliyense amanamiza mʼbale wake;

ndi pakamwa pawo pabodza amayankhula zachinyengo.

3Inu Yehova tsekani milomo yonse yachinyengo

ndi pakamwa paliponse podzikuza.

4Pakamwa pamene pamati, “Ife tidzapambana ndi kuyankhula kwathu;

pakamwapa ndi pathupathu, tsono mbuye wathu ndani?”

5“Chifukwa cha kuponderezedwa kwa anthu opanda mphamvu

ndi kubuwula kwa anthu osowa,

Ine ndidzauka tsopano,” akutero Yehova,

“Ndidzawateteza kwa owazunza.”

6Ndipo mawu a Yehova ndi angwiro

monga siliva oyengedwa mʼngʼanjo yadothi,

oyengedwa kasanu nʼkawiri.

7Inu Yehova mudzatitchinjiriza ndipo

mudzatiteteza kwa anthu otere kwamuyaya.

8Oyipa amangoyendayenda ponseponse

anthu akamayamikira zochita zawo.