KITABU CHA KWANZA
(Zaburi 1–41)
Zaburi 1
Furaha Ya Kweli
11:1 Kum 33:29; Za 40:4; 26:9; 37:38; 51:13; 104:35; 26:4; 10:2-11; 128:4; 89:15; 81:12; Mwa 49:6; Isa 28:14; Hos 7:5; Ay 21:16; 11:3; 31:5; Mit 1:22; 4:14Heri mtu yule ambaye
haendi katika shauri la watu waovu,
wala hasimami katika njia ya wenye dhambi,
au kuketi katika baraza la wenye mizaha.
21:2 Za 19:7; 119:1, 16, 35; 112:1; Rum 7:22; Eze 11:20; 18:17; Mwa 24:63Bali huifurahia sheria ya Bwana,
naye huitafakari hiyo sheria usiku na mchana.
31:3 Za 46:4; 65:9; 52:8; 92:12, 14; 128:2, 3; Yer 11:16; Zek 4:3; Hes 24:6; Ay 14:9; Eze 17:5; 47:12; Isa 1:30; 64:6; Mwa 39:3Mtu huyo ni kama mti uliopandwa
kando ya vijito vya maji,
ambao huzaa matunda kwa majira yake
na majani yake hayanyauki.
Lolote afanyalo hufanikiwa.
Huzuni Ya Waovu
41:4 Ay 13:25; Isa 40:24; Yer 13:24Sivyo walivyo waovu!
Wao ni kama makapi
yapeperushwayo na upepo.
51:5 Za 5:5; 26:12; 35:28; 82:1; 89:5; 107:32; 111:1; 149:1; Ay 19:29; 1:6; Za 37:18; 121:5; 145:20; 9:6; Nah 1:7; Law 26:38; Yn 1:41Kwa hiyo waovu hawatastahimili hukumu,
wala wenye dhambi katika kusanyiko la wenye haki.
6Kwa maana Bwana huziangalia njia za mwenye haki,
bali njia ya waovu itaangamia.
BUKU LOYAMBA
Masalimo 1–41
Salimo 1
1Wodala munthu
amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,
kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,
kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova
ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,
umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake
ndipo masamba ake safota.
Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
4Sizitero ndi anthu oyipa!
Iwo ali ngati mungu
umene umawuluzidwa ndi mphepo.
5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,
kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,
koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.