Zaburi 1 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Zaburi 1:1-6

KITABU CHA KWANZA

(Zaburi 1–41)

Zaburi 1

Furaha Ya Kweli

11:1 Kum 33:29; Za 40:4; 26:9; 37:38; 51:13; 104:35; 26:4; 10:2-11; 128:4; 89:15; 81:12; Mwa 49:6; Isa 28:14; Hos 7:5; Ay 21:16; 11:3; 31:5; Mit 1:22; 4:14Heri mtu yule ambaye

haendi katika shauri la watu waovu,

wala hasimami katika njia ya wenye dhambi,

au kuketi katika baraza la wenye mizaha.

21:2 Za 19:7; 119:1, 16, 35; 112:1; Rum 7:22; Eze 11:20; 18:17; Mwa 24:63Bali huifurahia sheria ya Bwana,

naye huitafakari hiyo sheria usiku na mchana.

31:3 Za 46:4; 65:9; 52:8; 92:12, 14; 128:2, 3; Yer 11:16; Zek 4:3; Hes 24:6; Ay 14:9; Eze 17:5; 47:12; Isa 1:30; 64:6; Mwa 39:3Mtu huyo ni kama mti uliopandwa

kando ya vijito vya maji,

ambao huzaa matunda kwa majira yake

na majani yake hayanyauki.

Lolote afanyalo hufanikiwa.

Huzuni Ya Waovu

41:4 Ay 13:25; Isa 40:24; Yer 13:24Sivyo walivyo waovu!

Wao ni kama makapi

yapeperushwayo na upepo.

51:5 Za 5:5; 26:12; 35:28; 82:1; 89:5; 107:32; 111:1; 149:1; Ay 19:29; 1:6; Za 37:18; 121:5; 145:20; 9:6; Nah 1:7; Law 26:38; Yn 1:41Kwa hiyo waovu hawatastahimili hukumu,

wala wenye dhambi katika kusanyiko la wenye haki.

6Kwa maana Bwana huziangalia njia za mwenye haki,

bali njia ya waovu itaangamia.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 1:1-6

BUKU LOYAMBA

Masalimo 1–41

Salimo 1

1Wodala munthu

amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa,

kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa,

kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.

2Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova

ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.

3Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi,

umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake

ndipo masamba ake safota.

Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.

4Sizitero ndi anthu oyipa!

Iwo ali ngati mungu

umene umawuluzidwa ndi mphepo.

5Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo,

kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.

6Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama,

koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.