Mithali 5 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Mithali 5:1-23

Onyo Dhidi Ya Uzinzi

15:1 Mit 1:8Mwanangu, sikiliza kwa makini hekima yangu,

sikiliza vizuri maneno yangu ya busara,

25:2 Mwa 2:7ili uweze kutunza busara

na midomo yako ihifadhi maarifa.

35:3 Za 55:21; Mit 2:16Kwa maana midomo ya mwanamke kahaba

hudondoza asali,

na maneno ya kinywa chake

ni laini kuliko mafuta;

45:4 Mhu 7:26; Ebr 4:12lakini mwisho wake ni mchungu kama nyongo,

mkali kama upanga ukatao kuwili.

55:5 Za 9:17; Mit 2:18Miguu yake hushuka kuelekea kwenye kifo;

hatua zake huelekea moja kwa moja kaburini.5:5 Kaburini hapa maana yake ni Kuzimu, kwa Kiebrania ni Sheol.

65:6 Mit 9:13; 30:20Yeye hafikiri juu ya njia ya uzima;

njia zake zimepotoka, lakini yeye hajui.

75:7 Mit 1:8-9Sasa basi wanangu, nisikilizeni;

msiache ninalowaambia.

85:8 Mit 6:20-29; 7:1-27Njia zenu ziwe mbali naye,

msiende karibu na mlango wa nyumba yake,

9usije ukatoa nguvu zako nzuri kwa wengine

na miaka yako kwa aliye mkatili,

105:10 Mit 29:3wageni wasije wakasherehekea utajiri wako

na jitihada yako ikatajirisha

nyumba ya mwanaume mwingine.

11Mwishoni mwa maisha yako utalia kwa uchungu,

wakati nyama na mwili wako vimechakaa.

12Utasema, “Tazama jinsi gani nilivyochukia adhabu!

Tazama jinsi moyo wangu ulivyodharau maonyo!

13Sikuwatii walimu wangu

wala kuwasikiliza wakufunzi wangu.

145:14 Mit 1:24-27; 6:33; 31:3Nimefika ukingoni mwa maangamizi kabisa

katikati ya kusanyiko lote.”

15Kunywa maji kutoka kwenye kisima chako mwenyewe,

maji yanayotiririka kutoka kwenye kisima chako mwenyewe.

16Je, chemchemi zako zifurike katika barabara za mji

na vijito vyako vya maji viwanjani?

17Na viwe vyako mwenyewe,

kamwe visishirikishwe wageni.

185:18 Wim 4:12-15; Kum 20:7; Mal 2:14Chemchemi yako na ibarikiwe

na umfurahie mke wa ujana wako.

195:19 Wim 2:9; 8:14Kulungu jike apendaye, kulungu mzuri:

matiti yake na yakutosheleze siku zote,

nawe utekwe daima na upendo wake.

205:20 Mit 2:16; 7:5Kwa nini mwanangu, utekwe na mwanamke kahaba?

Kwa nini ukumbatie kifua cha mke wa mwanaume mwingine?

215:21 Za 119:168; Hos 7:2; Yer 16:17; Ay 10:4; Ebr 4:13Kwa maana njia za mtu ni wazi kabisa mbele za Bwana,

naye huyapima mapito yake yote.

225:22 Za 9:16; Hes 32:23; Ay 18:9Matendo mabaya ya mtu mwovu humnasa yeye mwenyewe;

kamba za dhambi yake humkamata kwa nguvu.

235:23 Ay 4:21; 36:12Atakufa kwa kukosa nidhamu,

akipotoshwa kwa upumbavu wake mwenyewe.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Miyambo 5:1-23

Chenjezo kwa Mkazi Wachigololo

1Mwana wanga, mvetsera bwino za nzeru zimene ndikukuwuzazi,

tchera khutu ku mawu odziwitsa bwino zinthu ndikukupatsa,

2kuti uthe kuchita zinthu mochenjera ndi mwanzeru

ndiponso kuti utetezedwe ku mayankhulidwe a mkazi wachilendo.

3Pakuti mkazi wachigololo ali ndi mawu okoma ngati uchi.

Zoyankhula zake ndi zosalala ngati mafuta,

4koma kotsirizira kwake ngowawa ngati ndulu;

ngakuthwa ngati lupanga lakuthwa konsekonse.

5Mapazi ake amatsikira ku imfa;

akamayenda ndiye kuti akupita ku manda.

6Iye saganizirapo za njira ya moyo;

njira zake ndi zokhotakhota koma iye sadziwa izi.

7Tsopano ana inu, mundimvere;

musawasiye mawu anga.

8Uziyenda kutali ndi mkazi wotereyo,

usayandikire khomo la nyumba yake,

9kuopa kuti ungadzalanditse ulemerero wako kwa anthu ena;

ndi zaka zako kwa anthu ankhanza,

10kapenanso alendo angadyerere chuma chako

ndi phindu la ntchito yako kulemeretsa anthu ena.

11Potsiriza pa moyo wako udzabuwula,

thupi lako lonse litatheratu.

12Ndipo udzati, “Mayo ine, ndinkadana ndi kusunga mwambo!

Mtima wanga unkanyoza chidzudzulo!

13Sindinamvere aphunzitsi anga

kapena alangizi anga.

14Ine ndatsala pangʼono kuti ndiwonongeke

pakati pa msonkhano wonse.”

15Imwa madzi a mʼchitsime chakochako,

madzi abwino ochokera mʼchitsime chako.

16Kodi akasupe ako azingosefukira mʼmisewu?

Kodi mitsinje yako izingoyendayenda mʼzipata za mzinda?

17Mitsinjeyo ikhale ya iwe wekha,

osati uyigawireko alendo.

18Yehova adalitse kasupe wako,

ndipo usangalale ndi mkazi wa unyamata wako.

19Iye uja ali ngati mbalale yayikazi yokongola ndiponso ngati gwape wa maonekedwe abwino.

Ukhutitsidwe ndi mawere ake nthawi zonse,

ndipo utengeke ndi chikondi chake nthawi zonse.

20Mwana wanga, nʼchifukwa chiyani ukukopeka ndi mkazi wachigololo?

Bwanji ukukumbatira mkazi wachilendo?

21Pakuti mayendedwe onse a munthu Yehova amawaona,

ndipo Iye amapenyetsetsa njira zake zonse.

22Ntchito zoyipa za munthu woyipa zimamukola yekha;

zingwe za tchimo lake zimamumanga yekha.

23Iye adzafa chifukwa chosowa mwambo,

adzasocheretsedwa chifukwa cha uchitsiru wake waukulu.