11:1 Yer 26:18; 2Pet 1:21; 1Nya 3:12-13; Hos 1:1; Isa 1:1Neno la Bwana lilimjia Mika, Mmoreshethi, wakati wa utawala wa Yothamu, Ahazi na Hezekia, wafalme wa Yuda; ufunuo aliouona kuhusu Samaria na Yerusalemu.
21:2 Kum 4:26; 32:1; Yer 6:19; Mwa 31:50; Za 11:4; Isa 1:2Sikieni, enyi mataifa, enyi nyote,
sikilizeni, ee dunia na wote mliomo ndani yake,
ili Bwana Mwenyezi ashuhudie dhidi yenu,
Bwana kutoka Hekalu lake takatifu.
Hukumu Dhidi Ya Samaria Na Yerusalemu
31:3 Isa 18:4; 64:1; 26:21; Eze 3:12; Ebr 12:18, 19; Amo 4:13Tazama! Bwana anakuja kutoka mahali pake;
anashuka na kukanyaga
mahali palipoinuka juu pa dunia.
41:4 Za 46:2-6; Hes 16:31; Nah 1:5Milima inayeyuka chini yake
na mabonde yanagawanyika
kama nta mbele ya moto,
kama maji yatiririkayo kasi
kwenye mteremko.
51:5 Amo 8:14; Hos 5:5; Yer 2:18-19Yote haya ni kwa sababu ya kosa la Yakobo,
ni kwa sababu ya dhambi za nyumba ya Israeli.
Kosa la Yakobo ni lipi?
Je, sio Samaria?
Je, mahali pa juu pa Yuda pa kuabudia miungu ni nini?
Je, sio Yerusalemu?
61:6 Kum 20:6; Amo 5:11“Kwa hiyo nitaufanya Samaria kuwa lundo la kokoto,
mahali pa kuotesha mizabibu.
Nitayamwaga mawe yake katika bonde
na kuacha wazi misingi yake.
71:7 Eze 6:6; Kut 32:20; Kum 9:21; 23:17-18Sanamu zake zote
zitavunjwa vipande vipande;
zawadi zake zote za Hekalu
zitachomwa kwa moto;
nitaharibu vinyago vyake vyote.
Kwa kuwa alikusanya zawadi zake
kutokana na ujira wa kahaba,
nazo zitatumika tena
kulipa mishahara ya kahaba.”
Kulia Na Kuomboleza
81:8 Isa 15:3; 20:2Kwa ajili ya hili nitalia na kuomboleza;
nitatembea bila viatu na tena uchi.
Nitabweka kama mbweha
na kuomboleza kama bundi.
91:9 Yer 46:11; 10:19; 2Fal 18:13; Isa 3:26Kwa sababu jeraha lake halitibiki;
limekuja Yuda.
Limefika hasa kwenye lango la watu wangu,
hata Yerusalemu kwenyewe.
10Usiliseme hili huko Gathi;
usilie hata kidogo.
Huko Beth-le-Afra
gaagaa mavumbini.
111:11 Eze 23:29Piteni mkiwa uchi na wenye aibu,
ninyi mkaao Shafiri.
Wale waishio Saanani
hawatatoka nje.
Beth-Eseli iko katika maombolezo;
kinga yake imeondolewa kwako.
121:12 Yer 14:19; 40:2Wale waishio Marothi wanagaagaa kwa maumivu
wakingoja msaada,
kwa sababu maangamizi yamekuja
kutoka kwa Bwana,
hata katika lango la Yerusalemu.
131:13 Yos 10:3; Za 9:14Enyi mkaao Lakishi,
fungeni farasi kwenye magari ya vita.
Mlikuwa chanzo cha dhambi
kwa Binti Sayuni,
kwa kuwa makosa ya Israeli
yalikutwa kwako.
141:14 2Fal 16:8; Yos 15:44; Yer 15:18Kwa hiyo utaipa Moresheth-Gathi
zawadi za kuagana.
Mji wa Akzibu utaonyesha wazi udanganyifu
kwa wafalme wa Israeli.
151:15 Yos 15:44; 12:15Nitawaleteeni atakayewashinda
ninyi mnaoishi Maresha.
Yeye aliye utukufu wa Israeli
atakuja Adulamu.
161:16 Law 13:40; Ay 1:20; 2Fal 18:13; Amo 5:27; Kum 4:27Nyoeni nywele zenu katika kuomboleza
kwa ajili ya watoto wenu mnaowafurahia;
jifanyieni upara kama tai,
kwa kuwa watawaacha
na kwenda uhamishoni.
1Yehova anayankhula ndi Mika wa ku Moreseti pa nthawi ya ulamuliro wa Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a ku Yuda. Awa ndi masomphenya amene iye anaona onena za Samariya ndi Yerusalemu.
2Tamverani, inu anthu a mitundu yonse,
mvetsera iwe dziko lapansi ndi okhala mʼmenemo,
pakuti Ambuye Yehova achitira umboni wokutsutsani,
Ambuye akuyankhula ali mʼnyumba yake yopatulika.
Chiweruzo cha Samariya ndi Yerusalemu
3Taonani! Yehova akubwera kuchokera ku malo ake;
Iye akutsika ndipo akuponda pa malo okwera a dziko lapansi.
4Mapiri akusungunuka pansi pake,
ndipo zigwa zikugawikana
ngati phula pa moto,
ngati madzi ochokera mʼphiri.
5Zonsezi ndi chifukwa cha cholakwa cha Yakobo,
chifukwa cha machimo a nyumba ya Israeli.
Kodi cholakwa cha Yakobo nʼchiyani?
Kodi si Samariya?
Kodi malo achipembedzo a Yuda ndi ati?
Kodi si Yerusalemu?
6“Choncho Ine ndidzasandutsa Samariya kukhala bwinja,
malo odzalamo mphesa.
Miyala yake ndidzayitaya ku chigwa
ndipo ndidzafukula maziko ake.
7Mafano ake onse ndidzawaphwanyaphwanya;
mphatso zake zonse ndidzazitentha ndi moto;
ndidzawononga zifanizo zonse za milungu yake.
Popeza analandira mphatso zake kuchokera ku malipiro a akazi achiwerewere,
mphatsozonso zidzagwiritsidwa ntchito ndi ena ngati malipiro a akazi achiwerewere.”
Kulira ndi Kumva Chisoni
8Chifukwa cha zimenezi ine ndidzalira momvetsa chisoni;
ndidzayenda wopanda nsapato ndi wamaliseche.
Ndidzafuwula ngati nkhandwe
ndi kulira ngati kadzidzi.
9Pakuti chilonda cha Samariya nʼchosachizika;
chafika ku Yuda.
Chafika pa chipata chenicheni cha anthu anga,
mpaka mu Yerusalemu mwenimwenimo.
10Musanene zimenezi ku Gati;
musalire nʼkomwe.
Mugubuduzike mu fumbi
ku Beti-Leafura.
11Inu anthu okhala ku Safiro,
muzipita ku ukapolo muli amaliseche ndi amanyazi.
Iwo amene akukhala ku Zanaani
sadzatuluka.
Beti-Ezeli akulira mwachisoni;
chitetezo chake chakuchokerani.
12Anthu amene amakhala ku Maroti akubuwula ndi ululu,
akuyembekezera thandizo,
chifukwa Yehova wabweretsa tsoka,
lafika mpaka pa chipata cha Yerusalemu.
13Inu anthu okhala ku Lakisi
mangani akavalo ku magaleta.
Inu amene munayamba kuchimwitsa
mwana wamkazi wa Ziyoni,
pakuti zolakwa za Israeli
zinapezeka pakati panu.
14Chifukwa chake perekani mphatso zolawirana
ndi a ku Moreseti Gati.
Mzinda wa Akizibu udzaonetsa kunama
kwa mafumu a Israeli.
15Ndidzabweretsa mgonjetsi kudzalimbana ndi inu
okhala mu Maresa.
Ulemerero wa Israeli udzafika
ku Adulamu.
16Metani mipala mitu yanu kuonetsa kuti mukulirira
ana anu amene mumawakonda;
mudzichititse dazi ngati dembo,
pakuti anawo adzatengedwa pakati panu kupita ku ukapolo.