Ayubu 19 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Ayubu 19:1-29

Hotuba Ya Sita Ya Ayubu

Ayubu Anajibu: Najua Mkombozi Wangu Yu Hai

1Ndipo Ayubu akajibu:

219:2 1Sam 1:6; Za 6:2, 3; Ay 6:9; 13:25“Je, mtaendelea kunitesa mpaka lini,

na kuniponda kwa maneno yenu?

319:3 Mwa 31:7; Ay 20:3Mara kumi hizi mmenishutumu;

bila aibu mnanishambulia.

419:4 Ay 6:24; Za 19:12; Eze 18:4Kama ni kweli nimepotoka,

kosa langu ninabaki kuhusika nalo mwenyewe.

519:5 Za 38:16; 55:12; Mik 7:8Kama kweli mngejitukuza wenyewe juu yangu,

na kutumia unyonge wangu dhidi yangu,

619:6 Ay 6:29; 18:8; 10:3basi jueni kuwa Mungu amenitendea yaliyo mabaya,

naye amekokota wavu wake kunizunguka.

719:7 Ay 9:24; 30:20; Za 22:2; Hab 1:2-4“Ingawa ninalia, ‘Nimetendewa mabaya!’ sipati jibu;

ingawa ninaomba msaada, hakuna haki.

819:8 Mao 3:7; Hos 2:6; Mhu 6:4; Yer 14:19Yeye ameizuia njia yangu hivyo siwezi kupita;

ameyafunika mapito yangu na giza.

919:9 Ay 12:17; Za 89:39-44; Mao 5:16Amenivua heshima yangu,

na kuniondolea taji kichwani pangu.

1019:10 Ay 12:14; 7:6; 14:7Amenibomoa kila upande hadi nimeisha;

amelingʼoa tegemeo langu kama mti.

1119:11 Ay 16:9; 13:14Hasira yake imewaka juu yangu;

amenihesabu kuwa miongoni mwa adui zake.

1219:12 Ay 16:13; 16:10; 3:23Majeshi yake yananisogelea kwa nguvu;

yamenizingira,

yamepiga kambi kulizunguka hema langu.

1319:13 Ay 16:10-13; 30:12; Mt 26:56; 2Tim 4:16“Amewatenga ndugu zangu mbali nami;

wale tunaojuana nao wamefarakana nami kabisa.

1419:14 Ay 19:19; 2Sam 15:12; Ay 12:4; 16:20; Za 88:18; Yer 20:10; 38:22Watu wa jamaa yangu wamekwenda mbali;

rafiki zangu wamenisahau.

1519:15 Mwa 14:14; Mhu 2:7Wageni wangu na watumishi wangu wa kike wananiona kama mgeni;

wananitazama kama mgeni.

16Namwita mtumishi wangu, wala haitiki,

ingawa namwomba kwa kinywa changu mwenyewe.

1719:17 Za 38:5Pumzi ya kinywa changu ni kinyaa kwa mke wangu;

nimekuwa chukizo mno kwa ndugu zangu mwenyewe.

1819:18 2Fal 2:23; Ay 13:25Hata watoto wadogo hunidhihaki;

ninapojitokeza, hunifanyia mzaha.

1919:19 Za 38:11; 55:12-13; Ay 3:10Rafiki zangu wa moyoni wote wananichukia kabisa;

wale niwapendao wamekuwa kinyume nami.

2019:20 Ay 2:5Mimi nimebaki mifupa na ngozi tu;

nimeponea nikiwa karibu kufa.

2119:21 Ay 6:14; Amu 2:15; Ay 4:5; 10:3; Mao 3:1“Nihurumieni, rafiki zangu, kuweni na huruma,

kwa kuwa mkono wa Mungu umenipiga.

2219:22 Ay 13:25; 16:11; Mit 30:14; Isa 53:4Kwa nini mnanifuatia kama Mungu afanyavyo?

Hamtosheki kamwe na mwili wangu?

2319:23 Kut 17:16; Isa 30:8“Laiti maneno yangu yangewekwa kwenye kumbukumbu,

laiti kwamba yangeandikwa kwenye kitabu,

2419:24 Yer 17:1; Ay 16:18kwamba yangechorwa kwenye risasi kwa kifaa cha chuma,

au kuyachonga juu ya mwamba milele!

2519:25 Law 25:25; Mit 23:11; 1Sam 14:39; Ay 16:19Ninajua kwamba Mkombozi19:25 Au: Mtetezi. wangu yu hai,

naye kwamba mwishoni atasimama juu ya nchi.

2619:26 Hes 12:8; 1Yn 3:2Nami baada ya ngozi yangu kuharibiwa,

bado nikiwa na mwili huu nitamwona Mungu;

2719:27 Lk 2:30; Za 42:1; 63:1; 54:2mimi nitamwona kwa macho yangu mwenyewe:

mimi, wala si mwingine.

Tazama jinsi moyo wangu unavyomtamani sana!

28“Kama mkisema, ‘Tazama tutakavyomwinda,

maadamu mzizi wa tatizo uko ndani yake,’

2919:29 Ay 15:22; Za 58:11; Mhu 12:14ninyi wenyewe uogopeni upanga,

kwa kuwa ghadhabu italeta adhabu kwa upanga,

nanyi ndipo mtakapojua kwamba kuna hukumu.”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 19:1-29

Mawu a Yobu

1Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2“Kodi mudzakhala mukundizunza mpaka liti,

ndi kundilasa ndi mawu anuwo?

3Inuyo mwandinyoza kwambiri;

mwanditsutsa mopanda manyazi.

4Ngati ndi zoona kuti ine ndasochera,

cholakwachotu nʼchanga.

5Ngati ndithudi mukudziyika nokha pamwamba panga,

ndi kugwiritsa ntchito kunyozedwa kwanga polimbana nane,

6pamenepa dziwani kuti Mulungu wandilakwira

ndipo wandizinga ukonde wake.

7“Ngakhale ndifuwule kuti, ‘Akundizunza!’ Palibe wondiyankha;

ngakhale ndipemphe thandizo, palibe wondichitira zolungama.

8Mulungu wanditsekera njira yanga kotero sindingathe kudutsa;

waphimba njira zanga ndi mdima.

9Iye wandilanda ulemu wanga

ndipo wandivula chipewa chaufumu pamutu panga.

10Wandiphwanyaphwanya mbali zonse ndipo ndatheratu;

Iye wazula chiyembekezo changa ngati mtengo.

11Wandikwiyira ndipo

akundiyesa mmodzi mwa adani ake.

12Ankhondo ake akubwera kwa ine mwamphamvu,

akonzekera zodzalimbana nane

ndipo azungulira nyumba yanga.

13“Mulungu wandisiyanitsa ndi abale anga;

wasandutsa odziwana nane kukhala achilendo kwa ine.

14Abale anga andithawa;

abwenzi anga andiyiwala.

15Anthu odzacheza ku nyumba kwanga ndiponso antchito anga aakazi andisandutsa mlendo;

ndasanduka mlendo mʼmaso mwawo.

16Ndikayitana wa ntchito wanga, iye sandiyankha,

ngakhale ndikapempha ndi pakamwa panga sandichitira kanthu.

17Mpweya wanga umamunyansa mkazi wanga;

ndine chinthu chonyansa kwa abale anga a mimba imodzi.

18Inde, ngakhale ana amandinyoza;

akandiona amandinyodola.

19Anzanga onse apamtima amanyansidwa nane;

iwo amene ndinkawakonda andiwukira.

20Ndangotsala khungu ndi mafupa okhaokha;

ndapulumuka lokumbakumba.

21“Mvereni chisoni, inu abwenzi anga, mvereni chisoni,

pakuti dzanja la Mulungu landikantha.

22Chifukwa chiyani mukundilondola ngati Mulungu?

Kodi simunatope nalo thupi langa?

23“Aa, achikhala mawu anga analembedwa,

achikhala analembedwa mʼbuku,

24akanalembedwa pa mwala ndi chitsulo,

akanalembedwa pa thanthwe kuti sangathe kufufutidwa!

25Koma ndikudziwa kuti mpulumutsi wanga ali ndi moyo,

ndipo pa nthawi yomaliza adzabwera kudzanditeteza.

26Ndipo khungu langa litatha nʼkuwonongeka,

mʼthupi langa lomweli ndidzamuona Mulungu.

27Ine ndemwe ndidzamuona Iye

ndi maso angawa, ineyo, osati wina ayi.

Ndithu mtima wanga ukufunitsitsadi!

28“Koma inu mukuti, ‘Haa! Tingamuzunze bwanji,

popeza kuti zonsezi zaoneka chifukwa cha iye yemweyo?’

29Inu muyenera kuopa lupanga;

pakuti mkwiyo wake umalangadi ndi lupanga;

zikadzatero muzadziwa kuti chiweruzo chilipo ndithu.”