Amosi 2 – NEN & CCL

Kiswahili Contemporary Version (Neno: Bibilia Takatifu)

Amosi 2:1-16

12:1 Eze 25:8; Sef 2:8; 2Fal 3:27; Isa 16:6; 33:2Hili ndilo asemalo Bwana:

“Kwa dhambi tatu za Moabu,

hata kwa dhambi nne, sitaizuia ghadhabu yangu.

Kwa sababu alichoma mifupa ya mfalme wa Edomu,

ikawa kama chokaa.

22:2 Yer 48:7, 24; Ay 39:25; Yos 6:20Nitatuma moto juu ya Moabu

ambao utateketeza ngome za Keriothi.

Moabu ataanguka kwa ghasia kubwa

katikati ya vilio vya vita na mlio wa tarumbeta.

32:3 Hes 24:17; Za 2:10; Isa 40:23; Eze 25:8-11; Sef 2:8-9Nitamwangamiza mtawala wake

na kuwaua maafisa wake wote pamoja naye,”

asema Bwana.

42:4 Law 26:14; 2Sam 12:9, 10; 2Nya 36:14-17; Neh 1:7; Hos 12:2; Eze 9:11; Dan 9:11; 2Fal 17:19; Yer 6:19; 16:12; Isa 5:24; 9:16; 28:15; Kut 34:15Hili ndilo asemalo Bwana:

“Kwa dhambi tatu za Yuda,

hata kwa dhambi nne, sitaizuia ghadhabu yangu.

Kwa sababu wameikataa sheria ya Bwana

na hawakuzishika amri zake,

kwa sababu wamepotoshwa na miungu ya uongo,

miungu ambayo babu zao waliifuata.

52:5 Yer 17:27; Hos 8:14; 2Fal 25:9; Amo 3:11; 2Nya 36:19Nitatuma moto juu ya Yuda

ambao utateketeza ngome za Yerusalemu.”

Hukumu Juu Ya Israeli

62:6 Isa 29:21; Yoe 3:3; Amo 5:11, 12; 8:6Hili ndilo asemalo Bwana:

“Kwa dhambi tatu za Israeli,

hata kwa dhambi nne, sitaizuia ghadhabu yangu.

Wanawauza wenye haki kwa fedha,

na maskini kwa jozi ya viatu.

72:7 Eze 36:20; 22:11; Law 18:21; 20:3; Amo 8:4; 5:11-12; Rum 2:24; Isa 10:2Wanakanyaga juu ya vichwa vya maskini,

kama vile juu ya mavumbi ya nchi,

na kukataa haki kwa walioonewa.

Baba na mwanawe hushiriki msichana mmoja,

kwa hivyo hulinajisi Jina langu takatifu.

82:8 Kut 22:26; Hos 7:14; 1Kor 10:21; Hab 2:6; Amo 6:6; Kum 24:12-14Watu hulala kando ya kila madhabahu

juu ya nguo zilizowekwa rehani.

Katika nyumba ya mungu wao hunywa mvinyo

ulionunuliwa kwa fedha walizotozwa watu.

92:9 Hes 13:32; 21:23-26; Yos 10:12; Ay 18:16; Mal 4:1; Isa 10:33; Za 29:9“Nilimwangamiza Mwamori mbele yao,

ingawa alikuwa mrefu kama mierezi,

na mwenye nguvu kama mialoni.

Niliyaangamiza matunda yake juu

na mizizi yake chini.

102:10 Kut 6:6; 20:2; Hes 21:23; Yos 13:4; Amo 9:7; Kum 8:2; 2:7“Niliwapandisha toka Misri,

na nikawaongoza miaka arobaini jangwani

niwape nchi ya Waamori.

112:11 Kut 18:18; Yer 7:25; Hes 6:2-3; Amu 13:5Pia niliinua manabii kutoka miongoni mwa wana wenu

na Wanadhiri kutoka miongoni mwa vijana wenu.

Je, hii si kweli, enyi watu wa Israeli?”

asema Bwana.

122:12 Mdo 4:18; Isa 30:10; Yer 11:21; Amo 7:12-13; Mik 2:6“Lakini mliwafanya Wanadhiri kunywa mvinyo

na kuwaamuru manabii wasitoe unabii.

13“Sasa basi, nitawaponda

kama gari lipondavyo wakati limejazwa nafaka.

142:14 1Fal 20:11; Yer 9:23; Za 33:16; Ay 11:20; Isa 30:16-17Mkimbiaji hodari hatanusurika,

wenye nguvu wataishiwa nguvu zao,

na shujaa hataweza kuokoa maisha yake.

152:15 Eze 39:3; Kut 15:21; Zek 10:5; Mhu 9:11Mpiga upinde atakimbia,

askari wapiga mbio hawataweza kutoroka,

na mpanda farasi hataokoa maisha yake.

162:16 Yer 48:41Hata askari walio mashujaa sana

siku hiyo watakimbia uchi,”

asema Bwana.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amosi 2:1-16

1Yehova akuti,

“Chifukwa anthu a ku Mowabu akunka nachimwirachimwira,

Ine sindileka kuwalanga.

Popeza anatentha mafupa a mfumu ya ku Edomu,

mpaka kuwasandutsa phulusa,

2Ine ndidzatumiza moto pa Mowabu,

umene udzanyeketsa nyumba zaufumu za ku Keriyoti.

Mowabu adzafera pakati pa nkhondo yoopsa,

mʼkati mwa mfuwu wa nkhondo ndi kuliza malipenga.

3Ndidzawononga wolamulira wake

ndi kupha akuluakulu onse amene ali pamodzi ndi iye,”

akutero Yehova.

4Yehova akuti,

“Chifukwa anthu a ku Yuda akunka nachimwirachimwira,

Ine sindileka kuwalanga.

Popeza iwo akana lamulo la Yehova

ndipo sanasunge malangizo ake,

popeza asocheretsedwa ndi milungu yabodza,

milungu imene makolo awo ankayitsatira,

5Ine ndidzatumiza moto pa Yuda,

umene udzanyeketsa nyumba zaufumu za ku Yerusalemu.”

Chilango cha Anthu a ku Israeli

6Yehova akuti,

“Chifukwa anthu a ku Israeli akunka nachimwirachimwira,

Ine sindileka kuwalanga.

Iwo amagulitsa anthu olungama ndi siliva,

ndi osauka ndi nsapato.

7Amapondereza anthu osauka

ngati akuponda fumbi,

ndipo sawaweruza mwachilungamo anthu oponderezedwa.

Abambo ndi mwana wawo amagonana ndi mtsikana mmodzi yemweyo,

ndipo potero amanyozetsa dzina langa loyera.

8Anthuwo amakagonana mʼmbali mwa guwa lililonse la nsembe

pa zovala zimene anatenga ngati chikole.

Mʼnyumba ya mulungu wawo

amamweramo vinyo amene analipiritsa anthu pa milandu.

9“Ine ndinawononga Aamori pamaso pawo,

ngakhale iwo anali anthu ataliatali ngati mikungudza

ndiponso amphamvu ngati mitengo ya thundu.

Ndinawononga zipatso zawo

ndiponso mizu yawo.

10“Ine ndinakutulutsani ku Igupto,

ndipo ndinakutsogolerani mʼchipululu kwa zaka makumi anayi,

kudzakupatsani dziko la Aamori.

11Ine ndinawutsanso ena mwa ana ako kuti akhale aneneri,

ndi ena mwa anyamata ako kuti akhale anaziri.

Kodi si choncho, inu Aisraeli?”

akutero Yehova.

12“Koma inu munawamwetsa vinyo anaziri aja,

ndipo munalamula aneneri kuti asanenere.

13“Tsono Ine ndidzakupsinjani

monga imapsinjikira ngolo imene yadzaza ndi tirigu.

14Munthu waliwiro sadzatha kuthawa,

munthu wamphamvu sadzakhalanso ndi nyonga,

wankhondo sadzapulumutsa moyo wake.

15Munthu wa uta sadzalimbika,

msilikali wothamanga kwambiri sadzapulumuka,

ndipo wokwera pa akavalo sadzapulumutsa moyo wake.

16Ngakhale asilikali olimba mtima kwambiri

adzathawa ali maliseche pa tsikulo,”

akutero Yehova.