ኢዮብ 25 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

ኢዮብ 25:1-6

በልዳዶስ

1ሹሐዊውም በልዳዶስ እንዲህ ሲል መለሰ፤

2“ገዥነትና ግርማ የእግዚአብሔር ናቸው፤

በሰማይም ከፍታ ሥርዐትን ያደርጋል።

3ሰራዊቱ ሊቈጠር ይችላልን?

ብርሃኑስ የማይወጣው በማን ላይ ነው?

4ሰው በእግዚአብሔር ፊት ጻድቅ ይሆን ዘንድ፣

ከሴትስ የተወለደ ንጹሕ ይሆን ዘንድ ይችላልን?

5በፊቱ ጨረቃ እንኳ ብሩህ ካልሆነች፣

ከዋክብትም ንጹሓን ካልሆኑ፣

6ይልቁን ከብል የሚቈጠር የሰው ልጅ፣

ትል የሆነውማ ሰው ምንኛ ያንስ!”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 25:1-6

Mawu a Bilidadi

1Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,

Iye amakhazikitsa bata mu ufumu wake kumwambako.

3Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?

Kodi kuwala kwake sikuwalira ndani?

4Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?

Kodi munthu wobadwa mwa mayi angakhale wangwiro?

5Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,

ndipo nyenyezi sizitha kuwala pamaso pake,

6nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,

mwana wa munthu amene ali ngati nyongolotsi!”