አሞጽ 5 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

አሞጽ 5:1-27

የእስራኤል ሕዝብ ለንስሓ መጠራት

1የእስራኤል ቤት ሆይ፤ ስለ እናንተ የምደረድረውን ይህን የሙሾ ቃል ስሙ፤

2“ድንግሊቱ እስራኤል ወደቀች፤

ከእንግዲህም አትነሣም፤

በገዛ ምድሯ ተጣለች፤

የሚያነሣትም የለም።”

3ጌታ እግዚአብሔር እንዲህ ይላል፤

“አንድ ሺሕ ብርቱዎችን ለእስራኤል የምታዘምት ከተማ፣

አንድ መቶ ብቻ ይቀሯታል፤

አንድ መቶ ብርቱዎችን የምታዘምተውም፣

ዐሥር ብቻ ይቀሯታል።”

4እግዚአብሔር ለእስራኤል ቤት እንዲህ ይላል፤

“እኔን ፈልጉ፤ በሕይወትም ትኖራላችሁ።”

5ቤቴልን አትፈልጉ፤

ወደ ጌልገላ አትሂዱ፤

ወደ ቤርሳቤህም አትሻገሩ፤

ጌልገላ በርግጥ ትማረካለች፤

ቤቴልም እንዳልነበረች5፥5 ሐዘን ትሆናለችና።

6እግዚአብሔርን ፈልጉ፤

በሕይወትም ትኖራላችሁ፤

አለዚያ እንደ እሳት የዮሴፍን ቤት ያወድማል፤

እሳቱም ቤቴልን ይበላል፤ የሚያጠፋውም የለም።

7እናንት ፍትሕን ወደ መራርነት የምትለውጡ፣

ጽድቅንም ወደ ምድር የምትጥሉ ወዮላችሁ!

8ሰባቱን ከዋክብትና ኦሪዮንን የሠራ፣

ጨለማውን ወደ ንጋት ብርሃን የሚለውጥ፣

ቀኑን አጨልሞ ሌሊት የሚያደርግ፣

የባሕሩንም ውሃ ጠርቶ፣

በገጸ ምድር ላይ የሚያፈስስ፣

ስሙ እግዚአብሔር ነው፤

9እርሱ በብርቱው ላይ ድንገተኛ ጥፋትን፣

በተመሸገውም ከተማ ላይ ውድመትን ያመጣል።

10እናንተ በፍርድ አደባባይ

የሚገሥጻችሁን ትጠላላችሁ፤ እውነት የሚናገረውንም ትንቃላችሁ።

11እናንተ ድኻውን ትረግጣላችሁ፤

እህል እንዲሰጣችሁም ታስገድዱታላችሁ፤

ስለዚህ በተጠረበ ድንጋይ ቤት ብትሠሩም፣

በውስጡ ግን አትኖሩም፤

ባማሩ የወይን ተክል ቦታዎች ወይን ብትተክሉም፣

የወይን ጠጁን ግን አትጠጡም፤

12ኀጢአታችሁ ምንኛ ታላቅ እንደ ሆነ፣

በደላችሁም የቱን ያህል እንደ በዛ እኔ ዐውቃለሁና።

ጻድቁን ትጨቍናላችሁ፤

ጕቦም ትቀበላላችሁ፤

በፍርድ አደባባይም ከድኻው ፍትሕ ትነጥቃላችሁ።

13ስለዚህ አስተዋይ ሰው በእንዲህ ያለ ጊዜ ዝም ይላል፤

ቀኖቹ ክፉዎች ናቸውና።

14በሕይወት ትኖሩ ዘንድ፣

መልካሙን እንጂ ክፉውን አትፈልጉ፤

ከዚያ በኋላ እንደ ተናገራችሁት፣

የሰራዊት አምላክ እግዚአብሔር ከእናንተ ጋር ይሆናል።

15ክፉውን ጥሉ፤ መልካሙንም ውደዱ፤

በፍርድ አደባባይም ፍትሕን አታጓድሉ፤

ምናልባትም የሰራዊት አምላክ እግዚአብሔር

ለዮሴፍ ትሩፍ ይራራ ይሆናል።

16ስለዚህ ጌታ የሰራዊት አምላክ እግዚአብሔር እንዲህ ይላል፤

“በየመንገዱ ሁሉ ወየው ተብሎ ይለቀሳል፤

በአደባባዩም የሥቃይ ጩኸት ይሆናል፤

ገበሬዎች ለልቅሶ፣

አልቃሾችም ለዋይታ ይጠራሉ።

17በየወይኑ ዕርሻ ሁሉ ወየው ተብሎ ይለቀሳል፤

እኔ በመካከላችሁ ዐልፋለሁና፤”

ይላል እግዚአብሔር

የእግዚአብሔር ቀን

18የእግዚአብሔርን ቀን ለምትሹ፣

ለእናንተ ወዮላችሁ!

የእግዚአብሔርን ቀን ለምን ትሻላችሁ?

ያ ቀን ጨለማ ነው እንጂ ብርሃን አይደለም።

19ይህ ቀን አንድ ሰው ከአንበሳ ሲሸሽ፣

ድብ እንደሚያጋጥመው፣

ወደ ቤቱም ገብቶ፣ እጁን በግድግዳው

ላይ ሲያሳርፍ፣

እባብ እንደሚነድፈው ነው።

20የእግዚአብሔር ቀን ብርሃን ሳይሆን ጨለማ፣

የብርሃን ጸዳል የሌለው ድቅድቅ ጨለማ አይደለምን?

21“ዓመት በዓላችሁን ተጸይፌአለሁ፤

ጠልቼውማለሁ፤ ጉባኤዎቻችሁ ደስ አያሰኙኝም።

22የሚቃጠል መሥዋዕትና የእህል ቍርባን ብታቀርቡልኝም፣

እኔ አልቀበለውም፤

ከሠቡ እንስሶቻችሁ የኅብረት መሥዋዕት5፥22 የሰላም መሥዋዕት በመባል የሚታወቀው ነው። ብታቀርቡልኝም፣

እኔ አልመለከተውም።

23የዝማሬህን ጩኸት ከእኔ አርቅ፤

የበገናህንም ዜማ አልሰማም።

24ነገር ግን ፍትሕ እንደ ወንዝ፣

ጽድቅም እንደማይደርቅ ምንጭ ይፍሰስ።

25“የእስራኤል ቤት ሆይ፤ አርባ ዓመት በምድረ በዳ፣

መሥዋዕትንና ቍርባንን አቅርባችሁልኝ ነበርን?

26ለራሳችሁ የሠራችሁትን፣

የንጉሣችሁን ቤተ ጣዖት፣

የጣዖቶቻችሁን ዐምድ፣

የአምላካችሁን5፥26 ወይም ንጉሣችሁን ሱኮትን ከፍ ከፍ አደረጋችሁት እንዲሁም ጣዖታችሁን ቀይዋን የከዋክብት አማልክታችሁን፣ ሰብዓ ሊቃናት የሞሌክን ቤተ ጣዖት እንዲሁም የአምላካችሁን የሬፋንን ከዋክብት ከፍ አደረጋችሁ ይላሉ። ኮከብ አንሥታችሁ ተሸከማችሁ።

27ስለዚህ ከደማስቆ ወዲያ እንድትሰደዱ አደርጋችኋለሁ፤”

ይላል ስሙ የሰራዊት አምላክ የሆነ እግዚአብሔር

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amosi 5:1-27

Mawu Odandawulira Aisraeli

1Israeli, imva mawu awa, nyimbo ya maliro imene ndikuyimba za iweyo:

2“Namwali Israeli wagwa,

moti sadzadzukanso,

wasiyidwa mʼdziko lake lomwe,

popanda woti ndi kumudzutsa.”

3Ambuye Yehova akuti,

“Mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 1,000 amphamvu

udzatsala ndi anthu 100 okha;

mzinda umene udzapite ku nkhondo ndi anthu 100 amphamvu

udzatsala ndi anthu khumi okha basi.”

4Zimene Yehova akunena kwa nyumba ya Israeli ndi izi:

“Mundifunefune kuti mukhale ndi moyo;

5musafunefune Beteli,

musapite ku Giligala,

musapite ku Beeriseba.

Pakuti Giligala adzatengedwa ndithu kupita ku ukapolo,

ndipo Beteli adzawonongekeratu.”

6Funani Yehova kuti mukhale ndi moyo,

mukapanda kutero Iye adzatentha nyumba ya Yosefe ngati moto;

motowo udzawononga,

ndipo sipadzakhala wina wozimitsa motowo ku Beteli.

7Inu amene mumasandutsa chiweruzo cholungama kukhala chowawa

ndi kunyoza chilungamo.

8(Iye amene analenga nyenyezi za Nsangwe ndi Akamwiniatsatana,

amene amasandutsa mdima kuti ukhale mmawa

ndi kudetsa usana kuti ukhale usiku,

amene amayitana madzi a mʼnyanja

ndi kuwathira pa dziko lapansi,

Yehova ndiye dzina lake.

9Iyeyo amabweretsa chiwonongeko modzidzimutsa pa anthu amphamvu

ndi kuwononga mizinda yotetezedwa),

10inu mumadana ndi amene amadzudzula mʼbwalo la milandu

ndi kunyoza amene amanena zoona.

11Mumapondereza munthu wosauka

ndi kumukakamiza kuti akupatseni tirigu.

Nʼchifukwa chake, ngakhale mwamanga nyumba zamiyala yosema,

inuyo simudzakhalamo.

Ngakhale mwalima minda yabwino ya mphesa,

inu simudzamwa vinyo wake.

12Pakuti Ine ndikudziwa kuchuluka kwa zolakwa zanu

ndi kukula kwa machimo anu.

Inu mumapondereza anthu olungama ndi kulandira ziphuphu

ndipo anthu osauka simuwaweruza mwachilungamo mʼmabwalo anu amilandu.

13Nʼchifukwa chake pa nthawi yotere munthu wanzeru sayankhulapo kanthu,

popeza ndi nthawi yoyipa.

14Muyike mtima wanu pa zabwino osati pa zoyipa,

kuti mukhale ndi moyo.

Mukatero Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzakhala nanu,

monga mmene mumanenera kuti ali nanu.

15Mudane ndi zoyipa, mukonde zabwino;

mukhazikitse chiweruzo cholungama mʼmabwalo anu amilandu.

Mwina mwake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse adzachitira chifundo

anthu otsala a mʼbanja la Yosefe.

16Choncho izi ndi zimene Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, akunena:

“Mʼmisewu monse mudzakhala kulira mofuwula,

ndi kulira chifukwa cha kuwawa kwa masautso kudzakhala paliponse.

Adzayitana alimi kuti adzalire,

ndipo anthu odziwa maliridwe anthetemya adzalira mofuwula.

17Mʼminda yonse ya mpesa mudzakhala kulira kokhakokha,

pakuti Ine ndidzadutsa pakati panu,”

akutero Yehova.

Tsiku la Yehova

18Tsoka kwa inu amene mumalakalaka

tsiku la Yehova!

Chifukwa chiyani mumalakalaka tsiku la Yehova?

Tsikulo kudzakhala mdima osati kuwala.

19Lidzakhala ngati tsiku limene munthu pothawa mkango

amakumana ndi chimbalangondo,

ngati pamene munthu walowa mʼnyumba,

natsamira dzanja lake pa khoma

ndipo njoka nʼkuluma.

20Kodi tsiku la Yehova silidzakhala mdima osati kuwala,

mdima wandiweyani, popanda powala pena paliponse?

21“Ndimadana nawo masiku anu achikondwerero ndipo ndimawanyoza;

sindikondwera nayo misonkhano yanu.

22Ngakhale mupereke nsembe zopsereza ndi nsembe zachakudya,

Ine sindidzazilandira.

Ngakhale mupereke nsembe zabwino zachiyanjano,

Ine sindidzaziyangʼana nʼkomwe.

23Musandisokose nazo nyimbo zanu!

Sindidzamvetsera kulira kwa azeze anu.

24Koma chiweruzo cholungama chiyende ngati madzi,

chilungamo ngati mtsinje wosaphwa!

25“Kodi pa zaka makumi anayi zimene munakhala mʼchipululu muja

munkandibweretsera nsembe ndi zopereka, inu nyumba ya Israeli?

26Inu mwanyamula kachisi wa mfumu yanu,

ndi nyenyezi ija Kaiwani,

mulungu wanu,

mafano amene munadzipangira.

27Nʼchifukwa chake Ine ndidzakupititsani ku ukapolo, kutali kupitirira ku Damasiko,”

akutero Yehova, amene dzina lake ndi Mulungu Wamphamvuzonse.