መዝሙር 76 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 76:1-12

መዝሙር 76

ግርማው ለሚያስፈራው አምላክ የቀረበ ቅኔ

ለመዘምራን አለቃ፤ በበገናዎች፤ የአሳፍ መዝሙር ማሕሌት።

1እግዚአብሔር በይሁዳ ታወቀ፤

ስሙም በእስራኤል ታላቅ ነው።

2ድንኳኑ በሳሌም፣

ማደሪያውም በጽዮን ነው።

3በዚያም ተወርዋሪውን ፍላጻ፣

ጋሻንና ሰይፍን፣ ጦርንም ሰበረ። ሴላ

4አንተ ብርሃን ተላብሰህ ደምቀሃል፤

ግርማዊነትህም ከዘላለም ተራሮች ይልቃል።

5ልበ ሙሉ የሆኑት ተዘርፈዋል፤

አንቀላፍተውም ተኝተዋል፤

ከጦረኞቹም መካከል፣

እጁን ማንቀሳቀስ የቻለ የለም።

6የያዕቆብ አምላክ ሆይ፤ ከተግሣጽህ የተነሣ፣

ፈረስና ፈረሰኛው ጭልጥ ብለው ተኝተዋል።

7መፈራት ያለብህ አንተ ብቻ ነህ፤

በተቈጣህ ጊዜ ማን በፊትህ መቆም ይችላል?

8አንተ ፍርድን ከሰማይ አሰማህ፤

ምድርም ፈርታ ጸጥ አለች፤

9አምላክ ሆይ፤ ይህም የሆነው አንተ የምድር ጐስቋሎችን ለማዳን፣

ለፍርድ በተነሣህ ጊዜ ነው። ሴላ

10ሰውን ብትቈጣ እንኳ ለክብርህ ይሆናል፤

ከቍጣ የተረፉትንም ትገታቸዋለህ።76፥10 በሕዝብህ ላይ የምታወርደው ቍጣ ለክብርህ ይሆናል ወይም በቍጣውም መታሰቢያነት ራስህን ታስታጥቃለህ የሚሉ አሉ።

11ለአምላካችሁ ለእግዚአብሔር ተሳሉ፤ ስእለቱንም አግቡ፤

በእርሱ ዙሪያ ያሉ ሁሉ፣

አስፈሪ ለሆነው ለእርሱ እጅ መንሻ ያምጡ።

12እርሱ የገዦችን መንፈስ ይሰብራል፤

በምድር ነገሥታትም ዘንድ የተፈራ ነው።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 76:1-12

Salimo 76

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo la Asafu.

1Mulungu amadziwika mu Yuda;

dzina lake ndi lotchuka mu Israeli.

2Tenti yake ili mu Salemu,

malo ake okhalamo mu Ziyoni.

3Kumeneko Iye anathyola mivi yowuluka,

zishango ndi malupanga, zida zankhondo.

Sela

4Wolemekezeka ndinu,

wamphamvu kuposa mapiri amene ali ndi nyama zambiri.

5Anthu owuma mtima amagona atalandidwa chuma,

Iwowo amagona tulo tawo totsiriza;

palibe mmodzi wamphamvu

amene angatukule manja ake.

6Pa kudzudzula kwanu, Inu Mulungu wa Yakobo,

kavalo pamodzi ndi galeta zimakhala chete zitagona pansi.

7Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa.

Angathe kuyima pamaso panu ndani mukakwiya?

8Kuchokera kumwamba Inu munalengeza chiweruzo,

ndipo dziko linaopa ndi kukhala chete,

9pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze,

kupulumutsa onse osautsidwa mʼdziko.

Sela

10Zoonadi, ukali wanu pa anthu umakubweretserani matamando

ndipo opulumuka ku ukali wanu mumawasunga pafupi nanu.

11Chitani malumbiro kwa Yehova Mulungu wanu ndipo muwakwaniritse;

anthu onse omuzungulira abweretse mphatso

kwa Iye amene ayenera kuopedwa.

12Iye amaswa mzimu wa olamulira;

amaopedwa ndi mafumu a dziko lapansi.