መዝሙር 70 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 70:1-5

መዝሙር 70

የጭንቀት ጩኸት

70፥1-5 ተጓ ምብ – መዝ 40፥13-17

ለመዘምራን አለቃ፤ የዳዊት መዝሙር፤ ለመታሰቢያ።

1አምላክ ሆይ፤ ታድነኝ ዘንድ ዘንበል በል፤

እግዚአብሔር ሆይ፤ እኔን ለመርዳት ፍጠን።

2ሕይወቴን ለማጥፋት የሚሹ፣

ይፈሩ፤ ሁከትም ይምጣባቸው፤ የእኔን መጐዳት የሚመኙ፣

በውርደት ወደ ኋላቸው ይመለሱ።

3በእኔ ላይ፣ “ዕሠይ! ዕሠይ!” የሚሉ፣

ተሸማቅቀው ወደ ኋላ ይመለሱ።

4ነገር ግን የሚሹህ ሁሉ፣

በአንተ ሐሤት ያድርጉ፤ ደስም ይበላቸው፤

“ማዳንህን የሚወድዱ ሁሉ ሁልጊዜ፣

እግዚአብሔር ከፍ ይበል!” ይበሉ።

5እኔ ግን ምስኪንና ችግረኛ ነኝ፤

አምላክ ሆይ፤ ፈጥነህ ድረስልኝ፤

ረዳቴም፣ ታዳጊዬም አንተ ነህና፤

እግዚአብሔር ሆይ፤ አትዘግይ።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 70:1-5

Salimo 70

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho.

1Fulumirani Mulungu kundipulumutsa;

Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.

2Iwo amene akufunafuna moyo wanga

achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa;

onse amene akukhumba chiwonongeko changa

abwezedwe mopanda ulemu.

3Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,”

abwerere chifukwa cha manyazi awo.

4Koma onse amene akufunafuna Inu

akondwere ndi kusangalala mwa Inu;

iwo amene amakonda chipulumutso chanu

nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”

5Koma ine ndine wosauka ndi wosowa;

bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu.

Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga;

Inu Yehova musachedwe.