መዝሙር 4 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 4:1-8

መዝሙር 4

የሠርክ ጸሎት

ለመዘምራን አለቃ፤ በበገናዎች የሚዜም የዳዊት መዝሙር።

1የጽድቄ አምላክ ሆይ፤

በጠራሁህ ጊዜ መልስልኝ፤

ከጭንቀቴ አሳርፈኝ፤

ማረኝ፤ ጸሎቴንም ስማ።

2ሰዎች ሆይ፤ እስከ መቼ ድረስ ክብሬን ዝቅ4፥2 ወይም ወደ ራሳችሁ ታደርጋላችሁ?

እስከ መቼስ ድረስ ከንቱ ነገርን ትወድዳላችሁ? ሐሰትንስ4፥2 ወይም የሐሰት አማልክት ትሻላችሁ? ሴላ

3እግዚአብሔር ጻድቁን ለራሱ እንደ ለየ ዕወቁ፤

እግዚአብሔር ወደ እርሱ በተጣራሁ ጊዜ ይሰማኛል።

4ስትቈጡ ኀጢአት አትሥሩ፤

በዐልጋችሁም ላይ ሳላችሁ፣

ልባችሁን መርምሩ፤ ጸጥም በሉ። ሴላ

5የጽድቅን መሥዋዕት አቅርቡ፤

በእግዚአብሔርም ታመኑ።

6ብዙዎች፣ “አንዳች በጎ ነገር ማን ያሳየናል?” ይላሉ፤

እግዚአብሔር ሆይ፤ የፊትህ ብርሃን በላያችን ይብራ።

7ስንዴና አዲስ የወይን ጠጅ በብዛት ባመረቱ ጊዜ ከሚያገኙት ደስታ ይልቅ፣

አንተ ልቤን በታላቅ ሐሤት ሞልተኸዋል።

8በሰላም እተኛለሁ፤ አንቀላፋለሁም፤

እግዚአብሔር ሆይ፤ ያለ ሥጋት የምታሳድረኝ አንተ ብቻ ነህና።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 4:1-8

Salimo 4

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide.

1Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu,

Inu Mulungu wa chilungamo changa.

Pumulitseni ku zowawa zanga;

chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.

2Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi?

Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza?

Sela.

3Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika;

Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.

4Kwiyani koma musachimwe;

pamene muli pa mabedi anu,

santhulani mitima yanu ndi kukhala chete.

Sela

5Perekani nsembe zolungama

ndipo dalirani Yehova.

6Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?”

Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.

7Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu

kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.

8Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere,

pakuti Inu nokha, Inu Yehova,

mumandisamalira bwino.