መዝሙር 27 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 27:1-14

መዝሙር 27

ከእግዚአብሔር ጋር ያለው ሰው ድፍረት

የዳዊት መዝሙር።

1እግዚአብሔር ብርሃኔና መድኅኔ ነው፤

የሚያስፈራኝ ማን ነው?

እግዚአብሔር ለሕይወቴ ዐምባዋ ነው፤

ማንን እፈራለሁ?

2ሥጋዬን ይበሉ ዘንድ፣27፥2 ወይም ስሜን ሊያጠፉ

ክፉዎች ገፍተው በመጡ ጊዜ፣

ጠላቶቼና ባላጋራዎቼ በተነሡብኝ ጊዜ፣

እነርሱ ተሰነካክለው ወደቁ።

3ሰራዊት ቢከብበኝ እንኳ፣

ልቤ አይፈራም፤

ጦርነት ቢነሣብኝ እንኳ፣

ልበ ሙሉ ነኝ።

4እግዚአብሔርን አንዲት ነገር እለምነዋለሁ፤

እርሷንም እሻለሁ፤

ይኸውም በሕይወቴ ዘመን ሁሉ፣

በእግዚአብሔር ቤት እኖር ዘንድ፣

የእግዚአብሔርን ክብር ውበት አይ ዘንድ፣

በመቅደሱም ሆኜ አሰላስል ዘንድ ነው።

5በመከራ ቀን፣

በድንኳኑ ውስጥ ይሰውረኛልና፤

በድንኳኑም ጓዳ ይሸሽገኛል።

6በዚህ ጊዜ በዙሪያዬ ባሉ ጠላቶቼ ላይ፣

ራሴ ከፍ ከፍ ይላል፤

በድንኳኑም ውስጥ የእልልታ መሥዋዕት እሠዋለሁ፤

ለእግዚአብሔር እቀኛለሁ፤

እዘምርለታለሁም።

7እግዚአብሔር ሆይ፤ ድምፄን ከፍ አድርጌ ስጮኽ ስማኝ፤

ራራልኝ፤ ስማኝም።

8“ፊቴን ፈልጉ” ባልህ ጊዜ፤27፥8 ወይም ልቤ ሆይ፤ ለአንተ “ፊቴን” አለ

ልቤ፣ እግዚአብሔር ሆይ፤ ፊትህን እሻለሁ አለች።

9ፊትህን ከእኔ አትሰውር፤

ተቈጥተህ አገልጋይህን አታርቀው፤

መቼም ረዳቴ ነህና።

አዳኝ አምላኬ ሆይ፤

አትጣለኝ፤ አትተወኝም።

10አባቴና እናቴ ቢተዉኝ እንኳ፣

እግዚአብሔር ይቀበለኛል።

11እግዚአብሔር ሆይ፤ መንገድህን አስተምረኝ፤

ስለ ጠላቶቼም፣

በቀና መንገድ ምራኝ።

12ለጠላቶቼ ፍላጎት አሳልፈህ አትስጠኝ፤

የሐሰት ምስክሮች ተነሥተውብኛልና፣

ዐመፃ የሚረጩ ናቸው።

13የእግዚአብሔርን ቸርነት

በሕያዋን ምድር እንደማይ

ሙሉ እምነቴ ነው።

14እግዚአብሔርን ተስፋ አድርግ፤

አይዞህ፣ በርታ፤

እግዚአብሔርን ተስፋ አድርግ።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 27:1-14

Salimo 27

Salimo la Davide.

1Yehova ndiye kuwunika kwanga ndi chipulumutso changa;

ndidzaopa yani?

Yehova ndi linga la moyo wanga;

ndidzachita mantha ndi yani?

2Pamene anthu oyipa abwera kudzalimbana nane

kudzadya mnofu wanga,

pamene adani anga ndi achiwembu andithira nkhondo,

iwo adzapunthwa ndi kugwa.

3Ngakhale gulu lankhondo lindizinge,

mtima wanga sudzaopa.

Ngakhale nkhondo itayambika kulimbana nane,

ngakhale nthawi imeneyo, ine ndidzalimbika mtima.

4Chinthu chimodzi chokha chimene ndipempha kwa Yehova,

ichi ndi chimene ndidzachifunafuna:

kuti ndikhale mʼNyumba ya Yehova

masiku onse a moyo wanga,

ndi kuyangʼana kukongola kwa Yehova,

ndi kumufunafuna Iye mʼNyumba yake.

5Pakuti pa tsiku la msautso

Iye adzanditeteza mʼmalo ake okhalamo;

adzandibisa mʼkati mwa Nyumba yake

ndi kukhazika ine pamwamba pa thanthwe.

6Kotero mutu wanga udzakwezedwa

kuposa adani anga amene andizungulira;

pa Nyumba yake ndidzapereka nsembe ndi mfuwu wachimwemwe;

ndidzayimba nyimbo kwa Yehova.

7Imvani mawu anga pamene ndiyitana Inu Yehova

mundichitire chifundo ndipo mundiyankhe.

8Mtima wanga ukuti kwa Inu, “Funafuna nkhope yake!”

Nkhope yanu Yehova ndidzayifunafuna.

9Musandibisire nkhope yanu,

musamubweze mtumiki wanu mwamkwiyo;

mwakhala muli thandizo langa.

Musandikane kapena kunditaya,

Inu Mulungu Mpulumutsi wanga.

10Ngakhale abambo ndi amayi anga anditaya

Yehova adzandisamala.

11Phunzitseni njira yanu Inu Yehova,

munditsogolere mʼnjira yowongoka

chifukwa cha ondizunza.

12Musandipereke ku zokhumba za adani anga,

pakuti mboni zambiri zauka kutsutsana nane

ndipo zikundiopseza.

13Ine ndikutsimikiza mtima za zimenezi;

ndidzaona ubwino wa Yehova

mʼdziko la anthu amoyo.

14Dikirani pa Yehova;

khalani anyonga ndipo limbani mtima

nimudikire Yehova.