መዝሙር 149 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 149:1-9

መዝሙር 149

የድል መዝሙር

1ሃሌ ሉያ።149፥1 አንዳንዶች ከ9 ጭምር እግዚአብሔር ይመስገን ይላሉ።

ለእግዚአብሔር አዲስ ቅኔ ተቀኙ፤

ምስጋናውንም በቅዱሳን ጉባኤ ዘምሩ።

2እስራኤል በፈጣሪው ደስ ይበለው፤

የጽዮንም ልጆች በንጉሣቸው ሐሤት ያድርጉ።

3ስሙን በሽብሸባ ያመስግኑ፤ በከበሮና በመሰንቆ ይዘምሩለት።

4እግዚአብሔር በሕዝቡ ደስ ይለዋልና፤

የዋሃንንም በማዳኑ ውበት ያጐናጽፋል።

5ቅዱሳን በዚህ ክብር ይጓደዱ፤

በመኝታቸውም ላይ እልል እያሉ ይዘምሩ።

6የአምላክ ውዳሴ በአንደበታቸው፣

ባለ ሁለት ልሳን ሰይፍም በእጃቸው ይሁን፤

7በዚህ ሕዝቦችን ይበቀላሉ፤

ሰዎችንም ይቀጣሉ፤

8ነገሥታታቸውን በሰንሰለት፣

መኳንንታቸውንም በእግር ብረት ያስራሉ፤

9ይህም በእነርሱ ላይ የተጻፈውን ፍርድ ለመፈጸም ነው።

ለቅዱሳኑም ሁሉ ይህች ክብር ናት።

ሃሌ ሉያ።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 149:1-9

Salimo 149

1Tamandani Yehova.

Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,

matamando ake mu msonkhano wa oyera mtima.

2Israeli asangalale mwa mlengi wake;

anthu a ku Ziyoni akondwere mwa Mfumu yawo.

3Atamande dzina lake povina

ndi kuyimbira Iye nyimbo ndi tambolini ndi pangwe.

4Pakuti Yehova amakondwera ndi anthu ake;

Iye amaveka chipulumutso odzichepetsa.

5Oyera mtima asangalale mu ulemu wake

ndi kuyimba mwachimwemwe pa mabedi awo.

6Matamando a Mulungu akhale pakamwa pawo,

ndi lupanga lakuthwa konsekonse mʼmanja mwawo,

7kubwezera chilango anthu a mitundu ina,

ndi kulanga anthu a mitundu yonse,

8kumanga mafumu awo ndi zingwe,

anthu awo otchuka ndi unyolo wachitsulo,

9kuchita zimene zinalembedwa zotsutsana nawo

Uwu ndi ulemerero wa oyera mtima ake onse.

Tamandani Yehova.