መዝሙር 134 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 134:1-3

መዝሙር 134

የሠርክ መዝሙር

መዝሙረ መዓርግ።

1እናንት በሌሊት ቆማችሁ በእግዚአብሔር ቤት የምታገለግሉ፣

የእግዚአብሔር ባሪያዎች ሁላችሁ እግዚአብሔርን ባርኩ።

2በመቅደሱ ውስጥ እጆቻችሁን አንሡ፤

እግዚአብሔርንም ባርኩ።

3ሰማይንና ምድርን የሠራ እግዚአብሔር

ከጽዮን ይባርክህ።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 134:1-3

Salimo 134

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Bwerani, mutamande Yehova, inu atumiki onse a Yehova,

amene mumatumikira usiku mʼnyumba ya Yehova.

2Kwezani manja anu mʼmalo opatulika

ndipo mutamande Yehova.

3Yehova wolenga kumwamba ndi dziko lapansi,

akudalitseni kuchokera mʼZiyoni.