መዝሙር 121 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 121:1-8

መዝሙር 121

የእስራኤል ጠባቂ

መዝሙረ መዓርግ።

1ዐይኖቼን ወደ ተራሮች አነሣሁ፤

ረድኤቴ ከወዴት ይመጣል?

2ረድኤቴ ሰማይንና ምድርን ከፈጠረ፣

ከእግዚአብሔር ዘንድ ይመጣል።

3እግርህ እንዲሸራተት አይፈቅድም፤

የሚጠብቅህም አይተኛም።

4እነሆ፤ እስራኤልን የሚጠብቅ አይተኛም፤ አያንቀላፋምም።

5እግዚአብሔር ይጠብቅሃል፤

እግዚአብሔር በቀኝህ በኩል ይከልልሃል።

6ፀሓይ በቀን አያቃጥልህም፤

ጨረቃም በሌሊት ጕዳት አታመጣብህም።

7እግዚአብሔር ከክፉ ሁሉ ይጠብቅሃል፤

ነፍስህንም ይንከባከባታል።

8እግዚአብሔር ከአሁን ጀምሮ እስከ ዘላለም፣

መውጣትህንና መግባትህን ይጠብቃል።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 121:1-8

Salimo 121

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Ndikweza maso anga ku mapiri;

kodi thandizo langa limachokera kuti?

2Thandizo langa limachokera kwa Yehova,

wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.

3Sadzalola kuti phazi lako literereke;

Iye amene amakusunga sadzawodzera.

4Taonani, Iye amene amasunga Israeli

sadzawodzera kapena kugona.

5Yehova ndiye amene amakusunga;

Yehova ndiye mthunzi wako ku dzanja lako lamanja.

6Dzuwa silidzakupweteka nthawi ya masana,

kapena mwezi nthawi ya usiku.

7Yehova adzakuteteza ku zoyipa zonse;

adzasunga moyo wako.

8Yehova adzayangʼanira kutuluka kwako ndi kulowa kwako;

kuyambira tsopano mpaka muyaya.