መዝሙር 10 – NASV & CCL

New Amharic Standard Version

መዝሙር 10:1-18

መዝሙር 1010 መዝ 9 እና 10 በመጀመሪያው የጥንት ቅጅ ላይ አንጓዎች ተከታታይ ፊደላት ባሉት የዕብራይስጥ ሆህያት የሚጀምሩ እንዲሁም ጅማሬው ወይም መጨረሻው ትርጕም ዐዘል የሆነ አንድ ወጥ ግጥም ነበር በሰብዓ ሊቃናት ውስጥ ሁለቱ አንድ መዝሙር ናቸው።

ለፍትሕ የቀረበ ልመና

1እግዚአብሔር ሆይ፤ ለምን እንዲህ ርቀህ ቆምህ?

በመከራ ጊዜስ ለምን ድምፅህን አጠፋህ?

2ክፉዎች የተጨነቀውን በእብሪት ያሳድዳሉ፤

በወጠኑት ተንኰል ይጠመዱ።

3ክፉ ሰው በልቡ ምኞት ይኵራራል፤

ስግብግቡን ይባርካል፤ እግዚአብሔርንም ይዳፈራል።

4ክፉ ሰው ከትዕቢቱ የተነሣ እግዚአብሔርን አይፈልግም፤

በሐሳቡም ሁሉ አምላክ የለም፤

5መንገዱ ዘወትር የተሳካ ነው፤

ዕቡይ፣ ከሕግህም የራቀ ነው።

በመሆኑም በጠላቶቹ ላይ ያፌዛል።

6በልቡም፣ “ከስፍራዬ የሚነቀንቀኝ የለም፤

ከትውልድ እስከ ትውልድም መከራ አያገኘኝም” ይላል።

7አፉ መርገምን፣ ቅጥፈትንና ግፍን የተሞላ ነው፤

ሽንገላና ክፋት ከምላሱ ሥር ይገኛሉ።

8በየመንደሩ ሥርቻ ያደፍጣል፤

ንጹሓንን በሰዋራ ስፍራ ይገድላል።

ዐይኖቹንም በምስኪኖች ላይ ያነጣጥራል።

9በደኑ ውስጥ እንዳለ አንበሳ በስውር ያደባል፤

ረዳት የሌለውን ለመያዝ ያሸምቃል፤

ድኻውንም አፈፍ አድርጎ በወጥመዱ ይጐትታል።

10ምስኪኑም ይደቅቃል፤ ዐንገቱን ይደፋል፤

ያልታደለውም በክንዱ ሥር ይወድቃል።

11በልቡም፣ “እግዚአብሔር ረስቷል፤

ፊቱን ሸፍኗል፤ ፈጽሞም አያይም”

ይላል።

12እግዚአብሔር ሆይ ተነሥ፤ አምላክ ሆይ፤ ክንድህን አንሣ፤

ረዳት የሌላቸውንም አትርሳ።

13ክፉ ሰው በእግዚአብሔር ላይ ለምን ክፉ ይናገራል?

በልቡስ፣ “ስለ ሥራዬ አይጠይቀኝም”

ለምን ይላል?

14አንተ ግን መከራንና ሐዘንን ታያለህ፤

በእጅህም ዋጋ ለመክፈል ትመለከታለህ፤

ምስኪኑም ራሱን በአንተ ላይ ይጥላል፤

ለድኻ አደግም ረዳቱ አንተ ነህ።

15የክፉውንና የበደለኛውን ክንድ ስበር፤

የእጁንም ስጠው፤

ምንም እስከማይገኝ ድረስ።

16እግዚአብሔር ከዘላለም እስከ ዘላለም ንጉሥ ነው፤

ሕዝቦችም ከምድሩ ይጠፋሉ።

17እግዚአብሔር ሆይ፤ የተገፉትን ምኞት ትሰማለህ፤

ልባቸውን ታበረታለህ፤ ጆሮህንም ወደ እነርሱ ጣል ታደርጋለህ፤

18ከዐፈር የተፈጠረ ሰው ከእንግዲህ

እንዳያስጨንቃቸው፣

አንተ ለድኻ ዐደጉና ለተገፋው ትሟገታለህ።

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 10:1-18

Salimo 10

1Nʼchifukwa chiyani Yehova mwayima patali?

Chifukwa chiyani mukudzibisa nokha pa nthawi ya mavuto?

2Mwa kunyada kwake munthu woyipa asaka wofowoka,

amene akodwa mʼnjira zimene iye wakonza.

3Iye amatamandira zokhumba za mu mtima wake;

amadalitsa aumbombo ndi kuchitira chipongwe Yehova.

4Mwa kunyada kwake woyipa safunafuna Mulungu;

mʼmaganizo ake wonse mulibe malo a Mulungu.

5Zinthu zake zimamuyendera bwino;

iye ndi wamwano ndipo malamulo anu ali nawo kutali;

amanyogodola adani ake onse.

6Iye amadziyankhulira kuti, “Palibe chimene chidzandigwedeze.

Ndidzakhala wokondwa nthawi zonse ndipo sindidzakhala pa mavuto.”

7Mʼkamwa mwake mwadzaza matemberero, mabodza ndi zoopseza;

zovutitsa ndi zoyipa zili pansi pa lilime lake.

8Iye amabisalira anthu pafupi ndi midzi,

kuchokera pobisalapo amapha anthu osalakwa,

amayangʼanayangʼana mwachinsinsi anthu oti awawononge.

9Amabisalira anthu ngati mkango pa zitsamba.

Amabisalira kuti agwire anthu opanda mphamvu;

amagwira anthu opanda mphamvu ndi kuwakokera mu ukonde wake.

10Anthuwo amawapondaponda ndipo amakomoka;

amakhala pansi pa mphamvu zake.

11Iye amati mu mtima mwake, “Mulungu wayiwala,

wabisa nkhope yake ndipo sakuonanso.”

12Dzukani Yehova! Onetsani dzanja lanu Inu Mulungu.

Musayiwale anthu opanda mphamvu.

13Nʼchifukwa chiyani munthu woyipa amachitira chipongwe Mulungu?

Chifukwa chiyani amati mu mtima mwake,

“Iye sandiyimba mlandu?”

14Komatu Inu Mulungu, mumazindikira mavuto ndi zosautsa,

mumaganizira zochitapo kanthu.

Wovutikayo amadzipereka yekha kwa Inu pakuti

Inu ndi mthandizi wa ana amasiye.

15Thyolani dzanja la woyipitsitsa ndi la munthu woyipa;

muzengeni mlandu chifukwa cha zoyipa zake

zimene sizikanadziwika.

16Yehova ndi Mfumu kwamuyaya;

mitundu ya anthu idzawonongeka kuchoka mʼdziko lake.

17Mumamva Inu Yehova, zokhumba za osautsidwa;

mumawalimbikitsa ndipo mumamva kulira kwawo.

18Kuteteza ana amasiye ndi oponderezedwa,

ndi cholinga chakuti munthu amene ali wa dziko lapansi asaopsenso.