Yobu 18 – LCB & CCL

Luganda Contemporary Bible

Yobu 18:1-21

Birudaadi Ayanukula

1Awo Birudaadi Omusukusi n’ayanukula n’agamba nti,

2“Mulikomya ddi okufuulafuula ebigambo?

Muddeemu amagezi, tulyoke twogere.

318:3 Zab 73:22Lwaki tutwalibwa ng’ente

era ne tulowoozebwa okuba abasirusiru mu maaso gammwe?

418:4 Yob 13:14Ggwe eyeyuzayuza olw’obusungu,

abantu ensi bagiveeko ku lulwo, oba enjazi zive mu bifo byazo?

518:5 Yob 21:17; Nge 13:9; 20:20; 24:20“Ddala etabaaza y’omukozi w’ebibi ezikidde,

era n’omuliro gw’ekyoto kye tegukyayaka.

6Ekitangaala kivudde mu weema ye;

n’ettaala eri ku mabbali ge nayo ezikidde.

718:7 a Nge 4:12 b Yob 5:13 c Yob 15:6Amaanyi gamuwedde, ebigere bye tebikyali bya maanyi,

era enkwe ze, ze zimusuula.

818:8 Yob 22:10; Zab 9:15; 35:7Eky’amazima ebigere bye byamusuula mu kitimba

era n’atangatanga mu butimba.

9Omutego gumukwata ekisinziiro;

akamasu ne kamunyweeza.

10Omuguwa gumukwekerwa mu ttaka;

akatego kamulindirira mu kkubo lye.

1118:11 a Yob 15:21; Yer 6:25; 20:3 b Yob 20:8Entiisa emukanga enjuuyi zonna

era n’emugoba kigere ku kigere.

1218:12 Is 8:21Emitawaana gimwesunga;

ekikangabwa kirindiridde okugwa kwe.

1318:13 Zek 14:12Kirya ebitundu by’olususu lwe;

omubereberye wa walumbe amulyako emikono n’ebigere.

1418:14 Yob 8:22Aggyibwa mu bukuumi bwa weema ye

era n’atwalibwa eri kabaka w’ebikangabwa.

1518:15 Zab 11:6Omuliro gumalirawo ddala byonna eby’omu weema ye;

ekibiriiti kyakira mu kifo mw’abeera.

1618:16 a Is 5:24; Kos 9:1-16; Am 2:9 b Yob 15:30; Mal 4:1Emirandira gye gikala wansi,

n’amatabi ge gakala waggulu.

1718:17 Zab 34:16; Nge 2:22; 10:7Ekijjukizo kye kibula ku nsi;

talina linnya mu nsi.

1818:18 Yob 5:14Agobebwa okuva mu kitangaala, agenda mu kizikiza

n’aggyibwa mu nsi.

1918:19 a Yer 22:30 b Is 14:22 c Yob 27:14-15Talina mwana wadde omuzzukulu mu bantu be,

newaakubadde ekifo mwabeera.

2018:20 Zab 37:13; Yer 50:27, 31Abantu ab’ebugwanjuba beewuunya ebyamutuukako;

n’ab’ebuvanjuba ne bakwatibwa ekikangabwa.

2118:21 a Yob 21:28 b Yer 9:3; 1Bs 4:5Ddala bw’etyo bw’ebeera ennyumba y’omukozi w’ebibi;

bwe gaba bwe gatyo amaka g’oyo atamanyi Katonda.”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yobu 18:1-21

Mawu a Bilidadi

1Pamenepo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,

2“Kodi iwe Yobu utsiriza liti zoyankhula zakozi?

Khala munthu wozindikira zinthu ndipo ukatero ife tidzayankhula.

3Chifukwa chiyani ukutiyesa ngati ngʼombe

ndi kuoneka ngati opusa mʼmaso mwako?

4Iwe amene ukudzipweteka wekha ndi mkwiyo wako,

kodi dziko lapansi lisanduke bwinja chifukwa cha iweyo?

Kodi kapena thanthwe lisunthidwe kuchoka pa malo ake?

5“Nyale ya munthu woyipa yazimitsidwa;

malawi a moto wake sakuwalanso.

6Kuwala kwa mʼnyumba mwake kwasanduka mdima;

nyale ya pambali pake yazima.

7Mayendedwe ake amgugu azilala;

fundo zake zomwe zamugwetsa.

8Mapazi ake amulowetsa mu ukonde

ndipo akungoyendayenda mu ukondewo.

9Msampha wamkola mwendo;

khwekhwe lamugwiritsitsa.

10Amutchera msampha pansi mobisika;

atchera diwa pa njira yake.

11Zoopsa zikumuchititsa mantha kumbali zonse,

zikutsatira mayendedwe ake onse.

12Mphamvu zake zatha chifukwa cha njala,

tsoka likumudikira.

13Wagwidwa nthenda yoopsa thupi lonse;

miyendo yake, manja ake, zonse zawola.

14Wachotsedwa mʼnyumba imene ankadalira,

ndipo amukokera ku imfa, mfumu ya zoopsa zonse.

15Mʼnyumba mwake zonse zachotsedwamo;

awazamo sulufule kuti aphe tizirombo ta matenda.

16Mizu yake ikuwuma pansi

ndipo nthambi zake zikufota

17Sadzakumbukiridwanso pa dziko lapansi;

sadzakhalanso ndi chinthu chomutchukitsa mʼdziko.

18Amuchotsa pa malo owala ndi kumuponya ku mdima,

ndipo amupirikitsa pa dziko lonse.

19Iye alibe ana kapena zidzukulu pakati pa anthu ake,

kulibe wotsala kumene iye ankakhala.

20Anthu akumadzulo adabwa kwambiri ndi tsoka lake;

anthu akummawa agwidwa ndi mantha aakulu.

21Ndithudi, izi ndiye zimagwera munthu woyipa;

amenewa ndiye mathero a munthu amene sadziwa Mulungu.”