Ekyamateeka Olwokubiri 33 – LCB & CCL

Luganda Contemporary Bible

Ekyamateeka Olwokubiri 33:1-29

Musa Asabira Ebika bya Isirayiri Omukisa Omulundi gwe Ogwasembayo

133:1 Yos 14:6Guno gwe mukisa, Musa musajja wa Katonda gwe yasabira abaana ba Isirayiri nga tannafa. 233:2 a Kuv 19:18; Zab 68:8 b Bal 5:4 c Kbk 3:3 d Dan 7:10; Bik 7:53; Kub 5:11Yagamba nti,

Mukama Katonda yajja gye tuli ng’ava ku Sinaayi

n’atutuukako ng’ava ku Seyiri;

yamasamasa ng’ava ku Lusozi Palani.

Yajja n’obufukunya bw’abatukuvu

okuva ku bukiika obwaddyo obw’ensozi ze.

333:3 a Kos 11:1 b Ma 14:2 c Luk 10:39Mazima gw’oyagala abantu,

abatukuvu bonna bali mu mikono gyo.

Bavuunama wansi ku bigere byo

ne bawulira ebiragiro by’obawa.

433:4 a Yk 1:17 b Zab 119:111Ge mateeka Musa ge yatuwa

ng’ekyokufuna eky’ekibiina kya Yakobo.

5Waasitukawo kabaka mu Yesuluuni

abakulembeze b’abantu bwe baakuŋŋaana

nga bye bika bya Isirayiri ebyegasse.

6“Lewubeeni abenga mulamu; alemenga kuggwaawo

n’omuwendo gw’abasajja be gulemenga kukendeera.”

733:7 Lub 49:10Kino kye yayogera ku Yuda:

“Wulira, Ayi Mukama Katonda okukaaba kwa Yuda;

omuleete eri abantu be.

Yeerwaneko n’emikono gye.

Omuyambenga ng’alwanyisa abalabe be!”

833:8 a Kuv 28:30 b Kuv 17:7Bino bye yayogera ku Leevi:

“Sumimu wo ne Ulimu wo

biwe omusajja oyo gw’oyagala ennyo.

Wamukebera e Masa

n’omugezesa ku mazzi ag’e Meriba.

933:9 a Kuv 32:26-29 b Mal 2:5Yayogera ku kitaawe ne nnyina nti,

‘Abo sibafaako.’

Baganda be teyabategeeranga

wadde okusembeza abaana be;

baalabiriranga ekigambo kyo

ne bakuumanga endagaano yo.

1033:10 a Lv 10:11; Ma 31:9-13 b Zab 51:19Banaayigirizanga Yakobo ebiragiro byo

ne Isirayiri amateeka go.

Banaanyookezanga obubaane mu maaso go,

n’ebiweebwayo ebyokebwa ku kyoto kyo.

1133:11 2Sa 24:23Ayi Mukama Katonda owe omukisa byonna by’akola,

era okkirize emirimu gy’emikono gye.

Okubirenga ddala abo abamugolokokerako

okubenga abalabe be balemenga kwongera kumulumbanga.”

1233:12 a Ma 12:10 b Kuv 28:12Bye yayogera ku Benyamini:

“Omwagalwa wa Mukama Katonda abeerenga wanywevu,

Katonda Ali Waggulu ng’amwebulungudde bulijjo,

omwagalwa anaagalamiranga wakati ku bibegabega bye.”

1333:13 a Lub 49:25 b Lub 27:28Yayogera bw’ati ku Yusufu:

“Ettaka lye Mukama Katonda aliwe omukisa,

n’omusulo omulungi ennyo ogunaavanga waggulu mu ggulu

n’amazzi mu nzizi empanvu mu ttaka wansi,

14n’ebibala ebigimu ennyo ebinaavanga mu musana,

n’amakungula aganaasinganga mu myezi gyonna;

1533:15 Kbk 3:6n’ebibala ebinaakiranga obulungi ku nsozi ez’edda,

n’okwala kw’ebirime ku nsozi ez’emirembe gyonna;

1633:16 Kuv 3:2n’ebirabo ebisinga byonna mu nsi n’okujjula kwayo,

n’obuganzi obunaavanga eri oyo ow’omu kisaka ekyaka.

Ebyo byonna ka bijjenga ku mutwe gwa Yusufu,

mu kyenyi ky’omulangira mu baganda be.

1733:17 a Kbl 23:22 b 1Bk 22:11; Zab 44:5Mu kitiibwa anaabanga ente ennume embereberye

amayembe ge, ng’amayembe ga sseddume endalu;

anaagatomezanga amawanga n’agayuzaayuza,

n’agagoberanga ku nkomerero y’ensi.

Obwo bwe bunaabanga obukumi bwa Efulayimu

nga ze nkumi za Manase.”

1833:18 Lub 49:13-15Yayogera bw’ati ku Zebbulooni:

“Jaguzanga, ggwe Zebbulooni, bw’onoofulumanga;

ne Isakaali ng’ali mu weema zo.

1933:19 a Kuv 15:17; Is 2:3 b Zab 4:5 c Is 60:5, 11Banaakoowoolanga amawanga okwambuka ku nsozi

ne baweerangayo eyo ssaddaaka ez’obutuukirivu,

banaalyanga eby’obugagga ebya mayanja,

nga beeyambisa n’ebyobugagga ebikweke mu musenyu.”

2033:20 Lub 49:19Yayogera bw’ati ku Gaadi:

“Alina omukisa oyo agaziya ensalo z’omugabo gwa Gaadi,

Gaadi omwo mw’abeera ng’empologoma

ng’ayuza omukono n’omutwe.

2133:21 a Kbl 32:1-5, 31-32 b Yos 4:12; 22:1-3Yeerondera omugabo gw’ettaka erisinga obulungi,

omugabo gw’omukulembeze gwe gwamukuumirwa.

Abakulembeze b’abantu bwe baakuŋŋaana

ye yabasalira emisango gya Mukama,

n’okukwasa Isirayiri amateeka ga Mukama Katonda.”

2233:22 Lub 49:16Yayogera bw’ati ku Ddaani:

“Ddaani mwana gwa mpologoma,

ogubuuka nga guva mu Basani.”

23Yayogera bw’ati ku Nafutaali:

“Ggwe Nafutaali ajjudde obuganzi bwa Mukama Katonda

era ng’ojjudde emikisa gye,

onoosikira obukiikaddyo okutuuka ku nnyanja.”

2433:24 a Lub 49:21 b Lub 49:20; Yob 29:6Yayogera bw’ati ku Aseri:

“Asinga okuweebwa omukisa mu batabani ye Aseri,

ku baganda be gwe babanga basinga okwagala

era emizabbibu33:24 Waabangawo amafuta agaggibwanga mu mizabbibu, era amafuta ago kaali kabonero akalaga obugagga. gigimuke nnyo mu ttaka lye.

2533:25 Ma 4:40; 32:47Enzigi z’ebibuga byo zinaasibwanga n’eminyolo egy’ekyuma n’ekikomo

n’amaanyi go ganenkananga n’obuwangaazi bwo.

2633:26 a Kuv 15:11 b Zab 104:3“Tewali afaanana nga Katonda wa Yesuluuni

eyeebagala waggulu ku ggulu ng’ajja okukuyamba

ne ku bire mu kitiibwa kye.

2733:27 a Zab 90:1 b Yos 24:18 c Ma 7:2Katonda ataggwaawo bwe buddukiro bwo,

era akuwanirira n’emikono gye emirembe gyonna.

Anaagobanga abalabe bo nga naawe olaba,

n’agamba nti, ‘Bazikirize!’

2833:28 a Kbl 23:9; Yer 23:6 b Lub 27:28Bw’atyo Isirayiri anaabeeranga mu mirembe yekka,

ezzadde lya Yakobo linaabeeranga wanywevu,

mu nsi erimu emmere y’empeke ne wayini,

eggulu mwe linaatonnyezanga omusulo.

2933:29 a Zab 144:15 b Zab 18:44 c 2Sa 7:23 d Zab 115:9-11 e Ma 32:13Nga weesiimye, Ayi Isirayiri!

Ani akufaanana,

ggwe eggwanga Mukama Katonda lye yalokola?

Ye ngabo yo era omubeezi wo,

era kye kitala kyo ekisinga byonna.

Abalabe bo banaakuvuunamiranga,

era onoobalinnyiriranga.”

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Deuteronomo 33:1-29

Mose Adalitsa Mafuko a Aisraeli

1Awa ndi madalitso amene Mose, munthu wa Mulungu, anawapereka kwa Aisraeli asanafe. 2Iye anati:

“Yehova anabwera kuchokera ku Sinai

ndipo anatulukira kuchokera ku Seiri;

anawala kuchokera pa Phiri la Parani.

Iye anabwera ndi chiwunyinji cha angelo

kuchokera kummwera, moto woyaka uli mʼdzanja mwake.

3Ndithu ndinu amene mumakonda anthu anu;

opatulika ake onse ali mʼmanja mwake.

Onse amagwada pansi pa mapazi anu

kuchokera kwa inu amalandira malangizo,

4malamulo amene Mose anatipatsa,

chuma chopambana cha mtundu wa Yakobo.

5Iye anali mfumu ya Yesuruni

pamene atsogoleri a anthu anasonkhana,

pamodzi ndi mafuko a Israeli.

6“Lolani Rubeni akhale ndi moyo ndipo asafe,

anthu ake asachepe pa chiwerengero.”

7Ndipo ponena za Yuda anati:

“Inu Yehova, imvani kulira kwa Yuda;

mubweretseni kwa anthu ake.

Ndi manja ake omwe adziteteze yekha.

Inu khalani thandizo lake polimbana ndi adani ake!”

8Za fuko la Alevi anati:

“Tumimu wanu ndi Urimu ndi za

mtumiki wanu wokhulupirika.

Munamuyesa ku Masa;

munalimbana naye ku madzi a ku Meriba.

9Iye ananena za abambo ake ndi amayi ake kuti,

‘Sindilabadira za iwo.’

Sanasamale za abale ake

kapena ana ake,

koma anayangʼanira mawu anu

ndipo anateteza pangano lanu.

10Iye amaphunzitsa Yakobo malangizo anu

ndi malamulo anu kwa Israeli.

Amafukiza lubani pamaso panu

ndiponso amapereka nsembe zanu zonse zopsereza pa guwa lanu.

11Inu Yehova, dalitsani luso lake lonse

ndipo mukondwere ndi ntchito za manja ake.

Menyani adani awo mʼchiwuno

kanthani amene amuwukira kuti asadzukenso.”

12Za fuko la Benjamini anati:

“Wokondedwa wa Yehova akhale mwamtendere mwa Iye,

pakuti amamuteteza tsiku lonse,

ndipo amene Yehova amamukonda amawusa pa mapewa ake.”

13Za fuko la Yosefe anati:

“Yehova adalitse dziko lake

ndi mame ambiri ochokera kumwamba

ndiponso madzi ambiri ochokera pansi pa nthaka;

14ndi zinthu zambiri zimene zimacha ndi dzuwa

ndiponso ndi zokolola zabwino kwambiri zimene zimacha ndi mwezi uliwonse;

15ndi zipatso zabwino kwambiri zochokera mʼmapiri amakedzanawa

ndiponso zokolola zochuluka zochokera ku zitunda zakalekale;

16ndi mphatso zabwino kwambiri zochokera pa dziko lapansi ndi zonse zimene zili mʼmenemo

ndiponso kukoma mtima kwa Iye amene amakhala mʼchitsamba choyaka moto.

Madalitso onsewa akhale pa mutu pa Yosefe,

wapaderadera pakati pa abale ake.

17Ulemerero wake uli ngati ngʼombe yayimuna yoyamba kubadwa;

nyanga zake zili ngati za njati.

Ndi nyanga zakezo adzapirikitsa anthu a mitundu ina,

ngakhale iwo amene akukhala ku malekezero a dziko lapansi.

Nyanga zimenezi ndiye anthu miyandamiyanda a Efereimu;

nyanga zimenezi ndiye anthu 1,000 a Manase.”

18Za fuko la Zebuloni anati:

“Kondwera Zebuloni, pamene ukutuluka,

ndipo iwe, Isakara, kondwera mʼmatenti ako.

19Adzayitanira mitundu ya anthu kumapiri,

kumeneko adzaperekako nsembe zachilungamo;

kumeneko adzadyerera zinthu zochuluka zochokera ku nyanja,

chuma chobisika mu mchenga.”

20Za fuko la Gadi anati:

“Wodala amene amakulitsa malire a Gadi!

Gadi amakhala kumeneko ngati mkango,

kukhadzula mkono kapena mutu.

21Iye anadzisankhira dziko labwino kwambiri;

gawo la mtsogoleri anasungira iye.

Pamene atsogoleri a anthu anasonkhana,

anachita chifuniro cha Yehova molungama,

ndiponso malamulo onena za Israeli.”

22Za fuko la Dani anati:

“Dani ndi mwana wamkango,

amene akutuluka ku Basani.”

23Za fuko la Nafutali anati:

“Nafutali wadzaza ndi kukoma mtima kwa Yehova

ndipo ndi wodzaza ndi madalitso ake;

cholowa chake chidzakhala mbali ya kummwera kwa nyanja.”

24Za fuko la Aseri anati:

“Mwana wodalitsika kwambiri ndi Aseri;

abale ake amukomere mtima,

ndipo asambe mapazi ake mʼmafuta.

25Zotsekera za zipata zako zidzakhala za chitsulo ndi za mkuwa,

ndi mphamvu zako zidzakhala ngati masiku a moyo wako.

26“Palibe wina wofanana ndi Mulungu wa Yesuruni,

amene amakwera pa thambo kukuthandizani

ndiponso pa mitambo ya ulemerero wake.

27Mulungu wamuyaya ndiye pothawirapo pathu,

ndipo pa dziko lapansi amakusungani ndi mphamvu zosatha.

Adzathamangitsa patsogolo panu mdani wanu,

adzanena kuti, ‘Muwonongeni!’

28Motero Israeli adzakhala yekha mwamtendere;

zidzukulu za Yakobo zili pa mtendere

mʼdziko la tirigu ndi vinyo watsopano,

kumene thambo limagwetsa mame.

29Iwe Israeli, ndiwe wodala!

Wofanana nanu ndani

anthu opulumutsidwa ndi Yehova?

Iye ndiye chishango ndi mthandizi wanu

ndi lupanga lanu la ulemerero.

Adani ako adzakugonjera,

ndipo iwe udzapondereza pansi malo awo achipembedzo.”