시편 97 – KLB & CCL

Korean Living Bible

시편 97:1-12

하나님의 의로운 통치

1여호와께서 통치하신다.

땅아, 기뻐하라.

바다의 섬들아, 즐거워하라.

2구름과 흑암이 그를 두르고

의와 공평이 그 보좌의 기초이다.

3불이 그 앞에서 나와

그의 주변 대적들을 사른다.

4그의 번개가 세계를 비추니

땅이 그것을 보고 떠는구나.

5산들이 여호와 앞에서

양초같이 녹았으니

온 세상의 주가 되시는

여호와 앞이라네.

6하늘이 그의 의를 선포하므로

모든 민족이 그의 영광을 보았다.

7우상을 섬기며

무가치한 신들을 자랑하는 자들은

다 수치를 당하리라.

너희 모든 신들아,

여호와를 경배하라.

8여호와여, 주의 심판 때문에

시온 사람들이 기뻐하고

유다 성들이 즐거워합니다.

9여호와여, 주는 온 땅에서

가장 높으신 분이시며

그 어떤 신보다도

위대하신 분이십니다.

10여호와를 사랑하는 자들아

악을 미워하라.

그는 자기 백성의 생명을 지키시고

악한 자의 손에서 그들을 구하시며

11의로운 자에게 빛을 비추고

마음이 정직한 자에게

기쁨을 주신다.

12의로운 자들아,

여호와께서 행하신 일로 기뻐하고

그의 거룩한 이름을 찬양하라.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 97:1-12

Salimo 97

1Yehova akulamulira, dziko lapansi lisangalale;

magombe akutali akondwere.

2Mitambo ndi mdima waukulu zamuzungulira;

chilungamo ndi kuweruza molungama ndiwo maziko a mpando wake waufumu.

3Moto umapita patsogolo pake

ndi kunyeketsa amaliwongo kumbali zonse.

4Zingʼaningʼani zake zimawalitsa dziko lonse;

dziko lapansi limaona ndipo limanjenjemera.

5Mapiri amasungunuka ngati phula pamaso pa Yehova,

pamaso pa Ambuye a dziko lonse lapansi.

6Mayiko akumwamba amalengeza za chilungamo chake,

ndipo mitundu yonse ya anthu imaona ulemerero wake.

7Onse amene amalambira mafano osema amachititsidwa manyazi,

iwo amene amanyadira mafano;

mulambireni, inu milungu yonse!

8Ziyoni akumva ndipo akukondwera,

midzi ya Yuda ikusangalala

chifukwa cha maweruzo anu Yehova.

9Pakuti Inu Yehova ndi Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi;

ndinu wokwezeka kupambana milungu yonse.

10Iwo amene amakonda Yehova adane ndi zoyipa

pakuti Iye amayangʼanira miyoyo ya amene amamukhulupirira

ndipo amawapulumutsa mʼdzanja la anthu oyipa

11Kuwala kumafika pa anthu olungama,

ndi chimwemwe kwa olungama mtima.

12Kondwerani mwa Yehova Inu olungama

ndipo tamandani dzina lake loyera.