詩篇 56 – JCB & CCL

Japanese Contemporary Bible

詩篇 56:1-13

56

1-2神よ、私をあわれんでください。

敵の軍勢が、夜も昼も押し寄せて来ます。

尊大にも私に襲いかかって、

私を制圧しようとしています。

3-4恐れるとき、私はあなたに信頼します。

あなたの約束だけが頼りなのです。

神に信頼している私に、

ただの人間が手出しなどできるわけがありません。

5彼らはいつでも私のことばをねじ曲げ、

どうしたら私を傷つけることができるかと

考えているのです。

6彼らは計画を練り上げるために集まり、

道ばたに潜んでは、私をねらって待ち伏せています。

7彼らは思いどおりに事を運ぶつもりでいるでしょう。

主よ。彼らの思いのままにはさせないでください。

どうか、怒りを燃やし、

彼らを地面に打ちつけてください。

8あなたは、私が夜通し

寝返りを打っているのをご存じです。

あなたは、私の涙を一滴残さず、

びんにすくい集めてくださいました。

その一滴一滴は、余すところなく、

あなたの文書に記録されています。

9私が助けを呼び求めると、

その日のうちに戦況は変わり、敵は逃げ惑います。

私にわかっているのは、ただこの一事、

神が味方だということだけです。

10-11私は神への信頼を失いません。

ああ、神のすばらしいお約束!

人間ごときが何をしかけてこようと、私は恐れません。

そうです、神は約束を守ってくださるのです。

12神よ。あなたへの約束は、きっと果たします。

助けていただいたことを心から感謝しています。

13なぜなら、あなたは、

私が地上で御前を歩めるように、死から救い出し、

転ばないように支えてくださったからです。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 56:1-13

Salimo 56

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a “Njiwa pa Mtengo wa Thundu wa Kutali.” Mikitamu ya Davide, pamene Afilisti anamugwira ku Gati.

1Mundichitire chifundo Inu Mulungu, pakuti anthu akundithamangitsa kwambiri;

tsiku lonse akundithira nkhondo.

2Ondinyoza akundithamangitsa tsiku lonse,

ambiri akumenyana nane monyada.

3Ndikachita mantha

ndimadalira Inu.

4Mwa Mulungu, amene mawu ake ine ndimatamanda,

mwa Mulungu ine ndimadaliramo; sindidzachita mantha.

Kodi munthu amene amafa angandichite chiyani?

5Tsiku lonse amatembenuza mawu anga;

nthawi zonse amakonza zondivulaza.

6Iwo amakambirana, amandibisalira,

amayangʼanitsitsa mayendedwe anga

ndipo amakhala ndi chidwi chofuna kuchotsa moyo wanga.

7Musalole konse kuti athawe;

mu mkwiyo wanu Mulungu mugwetse mitundu ya anthu.

8Mulembe za kulira kwanga,

mulembe chiwerengero cha misozi yanga mʼbuku lanu.

Kodi zimenezi sizinalembedwe mʼbuku lanulo?

9Adani anga adzabwerera mʼmbuyo

pamene ndidzalirira kwa Inu.

Pamenepo ndidzadziwa kuti Mulungu ali ku mbali yanga.

10Mwa Mulungu amene mawu ake ndimawatamanda,

mwa Yehova amene mawu ake ndimawatamanda,

11mwa Mulungu ine ndimadalira ndipo sindidzachita mantha.

Kodi munthu angandichite chiyani?

12Ndiyenera kuchita zomwe ndinalumbira kwa Mulungu;

ndidzapereka nsembe zanga zachiyamiko kwa inu.

13Pakuti mwawombola moyo wanga ku imfa

ndi mapazi anga kuti ndingagwe,

kuti ndiyende pamaso pa Mulungu

mʼkuwala kwa moyo.