詩篇 110 – JCB & CCL

Japanese Contemporary Bible

詩篇 110:1-7

110

1主は、私の救い主にお告げになりました。

「わたしに代わって、天地を治めなさい。

わたしは敵を服従させ、あなたの前にひれ伏させよう。」

2主は、あなたが敵を支配するために、

エルサレムに強固な王座をお据えになりました。

3あなたのご威光が輝き渡ると、

民はきよい祭服をまとって、

喜んでやって来るでしょう。

あなたは朝露のように、日々新しい力を帯びられます。

4主は、こう誓われました。

「あなたが永遠に

メルキゼデクのような祭司であるという契約は

決して無効にはならない。」

5主はあなたのそばにいて、あなたを守られます。

神はご自身の御怒りの日に、

多くの国々の王を打ち倒されます。

6主は国々を罰し、指導者を全滅させ、

死体でいっぱいにされます。

7しかし、主は道のほとりの泉から水を飲み、

勢いを増されます。

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 110:1-7

Salimo 110

Salimo la Davide.

1Yehova akuwuza Mbuye wanga kuti,

“Khala ku dzanja langa lamanja

mpaka nditasandutsa adani ako

kukhala chopondapo mapazi ako.”

2Yehova adzakuza ndodo yamphamvu ya ufumu wako kuchokera mʼZiyoni;

udzalamulira pakati pa adani ako.

3Ankhondo ako adzakhala odzipereka

pa tsiku lako la nkhondo.

Atavala chiyero chaulemerero,

kuchokera mʼmimba ya mʼbandakucha,

udzalandira mame a unyamata wako.

4Yehova walumbira

ndipo sadzasintha maganizo ake:

“Ndiwe wansembe mpaka muyaya

monga mwa unsembe wa Melikizedeki.”

5Ambuye ali kudzanja lako lamanja;

Iye adzaponda mafumu pa tsiku la ukali wake.

6Adzaweruza anthu a mitundu ina,

adzadzaza dziko lapansi ndi mitembo ndipo adzaphwanya olamulira a pa dziko lonse lapansi.

7Iye adzamwa mu mtsinje wa mʼmbali mwa njira;

choncho adzaweramutsa mutu wake.