Psalmen 67 – HTB & CCL

Het Boek

Psalmen 67:1-8

1Een psalm voor de koordirigent. Een lied dat met snaarinstrumenten moet worden begeleid.

2Ik bid

dat God ons zijn genade zal geven

en ons zal zegenen.

Dat Hij Zichzelf aan ons zal openbaren.

3Dan zullen de mensen op aarde weten

wat uw wil is

en alle volken zullen door U worden bevrijd.

4Ik bid

dat alle volken U zullen loven en prijzen, o God,

dat zij werkelijk allemaal U zullen eren.

5Dat de volken zich in U zullen verheugen

en juichen zullen omdat U

elk volk rechtvaardig oordeelt

en uw weg wijst.

6Ik bid

dat alle volken U zullen loven en prijzen, o God,

dat zij werkelijk allemaal U de lof mogen brengen.

7Wij mochten een rijke oogst binnenhalen

omdat God, die onze God is, ons zo rijk zegent.

8God zegent ons

opdat de hele aarde

ontzag voor Hem heeft.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.