Psalm 125 – HOF & CCL

Hoffnung für Alle

Psalm 125:1-5

Auf Gottes Schutz ist Verlass!

1Ein Lied für Festbesucher, die nach Jerusalem hinaufziehen.

Wer dem Herrn vertraut, ist wie der Berg Zion;

er steht für immer unerschütterlich und fest.

2So wie sich die Berge rings um Jerusalem erheben –

so umgibt der Herr schützend sein Volk, jetzt und für alle Zeit.

3Nicht mehr lange werden gottlose Könige über unser Land herrschen,

das Gott denen zum Besitz gegeben hat, die ihm gehorchen.

Sonst könnten auch die noch dem Unrecht verfallen,

die sich bisher an seinen Willen hielten.

4Herr, tue denen Gutes, die Gutes tun,

denen, die aufrichtig mit dir leben!

5Diejenigen aber, die sich von dir abwenden und krumme Wege gehen,

wirst du verstoßen wie alle anderen Übeltäter!

Frieden komme über Israel!

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 125:1-5

Salimo 125

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni,

limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.

2Monga mapiri azungulira Yerusalemu,

momwemonso Yehova azungulira anthu ake

kuyambira tsopano mpaka muyaya.

3Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala

pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama,

kuti anthu olungamawo

angachite nawonso zoyipa.

4Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino,

amene ndi olungama mtima

5Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota,

Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa.

Mtendere ukhale pa Israeli.