Salmo 129 – CST & CCL

Nueva Versión Internacional (Castilian)

Salmo 129:1-8

Salmo 129

Cántico de los peregrinos.

1Mucho me han angustiado desde mi juventud

—que lo repita ahora Israel—,

2mucho me han angustiado desde mi juventud,

pero no han logrado vencerme.

3Sobre la espalda me pasaron el arado,

abriéndome en ella profundos129:3 profundos. Lit. largos. surcos.

4Pero el Señor, que es justo,

me libró de las ataduras de los impíos.

5Que retrocedan avergonzados

todos los que odian a Sión.

6Que sean como la hierba en el techo,

que antes de crecer se marchita;

7que no llena las manos del segador

ni el regazo del que cosecha.

8Que al pasar nadie les diga:

«La bendición del Señor sea con vosotros;

os bendecimos en el nombre del Señor».

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 129:1-8

Salimo 129

Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.

1“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,”

anene tsono Israeli;

2“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,

koma sanandipambane.

3Anthu otipula analima pa msana panga

ndipo anapangapo mizere yayitali:

4Koma Yehova ndi wolungama;

Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.”

5Onse amene amadana ndi Ziyoni

abwezedwe pambuyo mwamanyazi.

6Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba,

umene umafota usanakule;

7sungadzaze manja a owumweta

kapena manja a omanga mitolo.

8Odutsa pafupi asanene kuti,

“Dalitso la Yehova lili pa inu;

tikukudalitsani mʼdzina la Yehova.”