Salmo 129
Cántico de los peregrinos.
1Mucho me han angustiado desde mi juventud
—que lo repita ahora Israel—,
2mucho me han angustiado desde mi juventud,
pero no han logrado vencerme.
3Sobre la espalda me pasaron el arado,
abriéndome en ella profundos129:3 profundos. Lit. largos. surcos.
4Pero el Señor, que es justo,
me libró de las ataduras de los impíos.
5Que retrocedan avergonzados
todos los que odian a Sión.
6Que sean como la hierba en el techo,
que antes de crecer se marchita;
7que no llena las manos del segador
ni el regazo del que cosecha.
8Que al pasar nadie les diga:
«La bendición del Señor sea con vosotros;
os bendecimos en el nombre del Señor».
Salimo 129
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu.
1“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,”
anene tsono Israeli;
2“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,
koma sanandipambane.
3Anthu otipula analima pa msana panga
ndipo anapangapo mizere yayitali:
4Koma Yehova ndi wolungama;
Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.”
5Onse amene amadana ndi Ziyoni
abwezedwe pambuyo mwamanyazi.
6Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba,
umene umafota usanakule;
7sungadzaze manja a owumweta
kapena manja a omanga mitolo.
8Odutsa pafupi asanene kuti,
“Dalitso la Yehova lili pa inu;
tikukudalitsani mʼdzina la Yehova.”