Salmo 100 – CST & CCL

Nueva Versión Internacional (Castilian)

Salmo 100:1-5

Salmo 100

Salmo de acción de gracias.

1Aclamad alegres al Señor, habitantes de toda la tierra;

2adorad al Señor con regocijo.

Presentaos ante él

con cánticos de júbilo.

3Reconoced que el Señor es Dios;

él nos hizo, y somos suyos.100:3 y somos suyos (Targum, Qumrán y mss.); y no nosotros (TM).

Somos su pueblo, ovejas de su prado.

4Entrad por sus puertas con acción de gracias;

venid a sus atrios con himnos de alabanza;

dadle gracias, alabad su nombre.

5Porque el Señor es bueno y su gran amor es eterno;

su fidelidad permanece para siempre.

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 100:1-5

Salimo 100

Salimo. Nyimbo yothokoza.

1Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.

2Mulambireni Yehova mosangalala;

bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.

3Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.

Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake;

ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.

4Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko

ndi ku mabwalo ake ndi matamando;

muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.

5Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;

kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.