Salmo 100
Salmo de acción de gracias.
1Aclamad alegres al Señor, habitantes de toda la tierra;
2adorad al Señor con regocijo.
Presentaos ante él
con cánticos de júbilo.
3Reconoced que el Señor es Dios;
él nos hizo, y somos suyos.100:3 y somos suyos (Targum, Qumrán y mss.); y no nosotros (TM).
Somos su pueblo, ovejas de su prado.
4Entrad por sus puertas con acción de gracias;
venid a sus atrios con himnos de alabanza;
dadle gracias, alabad su nombre.
5Porque el Señor es bueno y su gran amor es eterno;
su fidelidad permanece para siempre.
Salimo 100
Salimo. Nyimbo yothokoza.
1Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2Mulambireni Yehova mosangalala;
bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
3Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu.
Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake;
ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
4Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko
ndi ku mabwalo ake ndi matamando;
muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
5Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya;
kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.