Yoswa 12 – CCL & NSP

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yoswa 12:1-24

Mayina a Mafumu Ogonjetsedwa

1Aisraeli anagonjetsa dziko lonse la kummawa kwa Yorodani, kuyambira ku chigwa cha Arinoni mpaka ku phiri la Herimoni pamodzi ndi dera lonse la kummawa kwa Araba. Iwo anatenga dzikoli kukhala lawo, ndipo mafumu a dzikoli anali awa:

2Sihoni mfumu ya Aamori,

amene ankakhala mu Hesiboni. Iye analamulira kuyambira ku Aroeri mzinda umene uli mʼmphepete mwa mtsinje wa Arinoni, mpaka ku mtsinje wa Yaboki, umene uli mʼmalire mwa Aamori, kuphatikizanso theka la dziko la Giliyadi. 3Iye ankalamuliranso dera la chigwa cha Yorodani kuyambira ku Nyanja ya Kinereti, kummawa ndi kumatsika mpaka ku Beti-Yesimoti, mzinda umene unali kummawa kwa Nyanja ya Mchere ndi kutsikabe kummwera mpaka pa tsinde pa phiri la Pisiga.

4Ogi mfumu ya mzinda wa Basani,

amene anali mmodzi mwa otsala mwa Arefaimu. Iye ankakhala ku Asiteroti ndi Ederi. 5Dera la ufumu wake linafika ku phiri la Herimoni, ku Saleka ndi dziko lonse la Basani mpaka ku malire ndi anthu a ku Gesuri Makati. Ufumu wake unaphatikizanso theka la Giliyadi mpaka ku malire a mfumu Sihoni ya ku Hesiboni.

6Mose mtumiki wa Yehova ndi Aisraeli anawagonjetsa ndipo anapereka dziko lawo kwa anthu a fuko la Rubeni, fuko la Gadi ndi theka la fuko la Manase kuti chikhale cholowa chawo.

7Yoswa ndi Aisraeli onse anagonjetsa mafumu onse okhala kumadzulo kwa mtsinje wa Yorodani kuyambira ku Baala-Gadi, ku chigwa cha Lebanoni mpaka ku phiri la Halaki, kumapita cha ku Seiri. Yoswa anagawira dzikolo mafuko a Israeli kuti likhale cholowa chawo. 8Dziko limeneli linali dera la ku mapiri, chigwa cha kumadzulo, chigwa cha Yorodani, ku matsitso a kummawa, ndi dziko la chipululu la kummwera. Amene ankakhala mʼdzikoli anali Ahiti, Aamori, Akanaani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi. Mafumu ake anali awa:

9mfumu ya Yeriko imodzimfumu ya Ai (kufupi ndi Beteli imodzi10mfumu ya Yerusalemu imodzimfumu ya Hebroni imodzi11mfumu ya Yarimuti imodzimfumu ya Lakisi imodzi12mfumu ya Egiloni imodzimfumu ya Gezeri imodzi13mfumu ya Debri imodzimfumu ya Gederi imodzi14mfumu ya Horima imodzimfumu ya Aradi imodzi15mfumu ya Libina imodzimfumu ya Adulamu imodzi16mfumu ya Makeda imodzimfumu ya Beteli imodzi17mfumu ya Tapuwa imodzimfumu ya Heferi imodzi18mfumu ya Afeki imodzimfumu ya Lasaroni imodzi19mfumu ya Madoni imodzimfumu ya Hazori imodzi20mfumu ya Simuroni Meroni imodzimfumu ya Akisafu imodzi21mfumu ya Taanaki imodzimfumu ya Megido imodzi22mfumu ya Kadesi imodzimfumu ya Yokineamu ku Karimeli imodzi23mfumu ya Dori ku Nafoti Dori imodzimfumu ya Goyini ku Giligala imodzi24mfumu ya Tiriza imodzimafumu onse pamodzi analipo 31.

New Serbian Translation

Књига Исуса Навина 12:1-24

Попис поражених царева

1А ово су цареви крајева које су Израиљци поразили, и освојили њихове земље с оне стране Јордана ка истоку, од потока Арнона до горе Ермон, са свом Арабом на истоку:

2Сихон, цар аморејски, који је столовао у Есевону;

његова владавина се простирала од Ароира, који лежи на рубу потока Арнона, средином потока и половином Галада све до потока Јавока, који чини границу са Амонцима,

3обухватајући источну Араву до језера Хинерет, све до Арапског или Мртвог мора у правцу Вет-Јесимота на истоку, и обронака Фасге на југу.

4Затим, Ог цар васански; један од последњих Рефаимаца, који је столовао у Астароту и Едрајину.

5Његова владавина се простирала над гором Ермон, над Салком и над читавим Васаном до гесурске и махатске границе, и над половином Галада све до границе Сихона, есевонскога цара.

6Њих су Мојсије, слуга Господњи, и Израиљци побили, а ту земљу је Мојсије, слуга Господњи, дао у посед Рувимовом и Гадовом племену и половини Манасијиног племена.

7Ово су цареви земаља које су Исус и Израиљци поразили на западној страни Јордана, од Вал-Гада, у долини Ливана до горе Алака, што води горе у Сир. Исус је дао њихову земљу у посед Израиљевим племенима према њиховим деловима, 8у горју, у равници, Арави, по обронцима, у пустињи, у Негеву: земљу Хетита, Аморејаца, Хананаца, Фережана, Евејаца, и Јевусејаца:

9цар јерихонски, један;

цар гајски (код Ветиља), један;

10цар јерусалимски, један;

цар хевронски, један;

11цар јармутски, један;

цар лахиски, један;

12цар еглонски, један;

цар гезерски, један;

13цар давирски, један;

цар гадерски, један;

14цар орматски, један;

цар арадски, један;

15цар ливњански, један;

цар одоламски, један;

16цар македски, један;

цар ветиљски, један;

17цар тафујшки, један;

цар еферски, један;

18цар афечки, један;

цар саронски, један;

19цар мадонски, један;

цар асорски, један;

20цар симрон-меронски, један;

цар ахсафски, један;

21цар танашки, један;

цар мегидски, један;

22цар кедески, један;

цар јокнеамски на Кармилу, један;

23цар дорски, у Нафат-Дору, један;

цар гојимски у Галгалу, један;

24цар терски, један.

Све укупно тридесет један цар.