Uthenga Wabwino wa Yehova
1Mzimu wa Ambuye Yehova uli pa ine,
chifukwa Yehova wandidzoza
kuti ndilalikire uthenga wabwino kwa anthu osauka.
Wandituma kuti ndikatonthoze anthu osweka mtima,
ndikalengeze kwa akapolo kuti alandire ufulu
ndiponso kuti ndikamasule a mʼndende.
2Wandituma kuti ndikalengeze nthawi imene Yehova adzapulumutsa anthu ake;
za tsiku limene Yehova adzalanga adani a anthu ake.
Wandituma kuti ndikatonthoze olira.
3Wandituma kuti ndiwakonzere olira a ku Ziyoni,
nkhata ya maluwa yokongola
mʼmalo mwa phulusa,
ndiwapatse mafuta achikondwerero
mʼmalo mwa kulira.
Ndiwapatse chovala cha matamando
mʼmalo mwa mtima wopsinjika.
Ndipo iwo adzatchedwa mitengo ya thundu yamphamvu yachilungamo,
yoyidzala Yehova
kuti Iye mwini apezemo ulemerero wake.
4Adzamanganso mabwinja akale a mzinda
ndipo malo amene anawonongeka kalekale aja adzakonzanso.
Adzakonzanso mizinda imene inapasuka,
imene yakhala yowonongeka kwa nthawi yayitali kwambiri.
5Anthu achilendo adzakutumikirani; adzazidyetsa ziweto zanu;
iwo adzagwira ntchito mʼminda yanu ya mpesa.
6Ndipo inu mudzatchedwa ansembe a Yehova,
adzakutchulani kuti ndinu atumiki a Mulungu wathu.
Mudzadyerera chuma cha mitundu ya anthu,
ndipo mudzanyadira ulemu umene mwalandira.
7Chifukwa manyazi awo anali owirikiza;
ndi kuti munalandira
chitonzo ndi kutukwana,
adzakondwera ndi cholowa chawo,
tsono adzalandira cholowa chawo cha chigawo cha dziko mowirikiza,
ndipo chimwemwe chamuyaya chidzakhala chawo.
8“Pakuti Ine Yehova, ndimakonda chilungamo;
ndimadana ndi zakuba ndi zoyipa.
Anthu anga ndidzawapatsa mphotho mokhulupirika
ndikupangana nawo pangano losatha.
9Ana awo adzakhala odziwika pakati pa mitundu ya anthu
ndipo adzukulu awo adzakhala otchuka pakati pa anthu a mitundu ina.
Aliyense wowaona adzazindikira
kuti ndi anthu amene Yehova wawadalitsa.”
10Ine ndikusangalala kwambiri chifukwa cha Yehova;
moyo wanga ukukondwera chifukwa cha Mulungu wanga.
Pakuti Iye wandiveka zovala zachipulumutso,
ndipo wandiveka mkanjo wachilungamo.
Zili ngati mkwati wovala nkhata ya maluwa mʼkhosi mwake,
ndiponso ngati mkwatibwi wovala mikanda yamtengowapatali.
11Monga momwe nthaka imameretsa mbewu
ndiponso monga munda umakulitsa mbewu zimene anadzala,
momwemonso Ambuye Yehova adzaonetsa chilungamo ndi matamando
pamaso pa mitundu yonse ya anthu.
Amawulire Amalungi ag’Obulokozi
161:1 a Is 11:2 b Zab 45:7 c Mat 11:5; Luk 7:22 d Is 57:15 e Is 42:7; 49:9Omwoyo wa Mukama Katonda ali ku nze,
kubanga Mukama anfuseeko amafuta okubuulira abaavu n’abali obubi ebigambo ebirungi,
antumye okuyimusa abalina emitima egimenyese.
Okulangirira eddembe eri abawambe,
n’abasibe bateebwe
bave mu makomera.
261:2 a Is 49:8; Luk 4:18-19* b Is 34:8 c Is 57:18; Mat 5:4Okulangirira omwaka gwa Mukama
ogw’okulabiramu obulungi bwe;
olunaku lwa Mukama olw’okuwalanirako eggwanga
era n’okuzzaamu amaanyi abo bonna abakungubaga.
361:3 Is 60:20-21Okugabirira abo bonna abali mu Sayuuni abakungubaga,
okubawa engule ey’obubalagavu mu kifo ky’evvu,
n’amafuta ag’essanyu mu kifo ky’ennaku.
Ekyambalo ky’okutendereza
mu kifo ky’omwoyo w’okukeŋŋeentererwa
balyoke bayitibwe miti gy’abutuukirivu, ebisimbe bya Mukama,
balyoke baweebwe ekitiibwa.
461:4 Is 49:8; Ez 36:33; Am 9:14Baliddamu
bazimbe ebyali bizise,
balirongoosa ebibuga
ebyali byerabirwa edda.
561:5 Is 14:1-2Abaamawanga balibalundira ebisibo byammwe,
abagwira babakolere mu nnimiro zammwe ne mu nnimiro z’emizabbibu.
661:6 a Kuv 19:6; 1Pe 2:5 b Is 60:11Era muyitibwe bakabona ba Mukama,
abantu baliboogerako ng’abaweereza ba Mukama,
mulirya obugagga bw’amawanga,
era mu bugagga bwabwe mwe mulyenyumiririza.
761:7 Is 40:2; Zek 9:12Mu kifo ky’ensonyi,
abantu bange baliddizibwawo emirundi ebiri.
Mu kifo ky’okuswala
basanyuke olw’ebyo bye balifuna
era balifuna omugabo gwa mirundi ebiri,
essanyu lyabwe liribeerera emirembe gyonna.
861:8 a Zab 11:7; Is 5:16 b Is 55:3“Kubanga nze, Mukama, njagala obwenkanya,
nkyawa okunyaga era n’obutali butuukirivu.
Mu bwesigwa bwange ndibasasula
era nkole nabo endagaano ey’emirembe n’emirembe.
9N’ezzadde lyabwe liritutumuka nnyo mu mawanga
n’abaana baabwe eri abantu.
Abo bonna abalibalaba balibamanya,
nti bantu Mukama be yawa omukisa.”
1061:10 a Is 25:9; Kbk 3:18 b Zab 132:9; Is 52:1 c Is 49:18; Kub 21:2Nsanyukira nnyo mu Mukama,
emmeeme yange esanyukira mu Katonda wange.
Kubanga annyambazizza ebyambalo eby’obulokozi
era n’anteekako n’omunagiro ogw’obutuukirivu,
ng’omugole omusajja bw’ayambala engule nga kabona,
ng’omugole omukazi bw’ayambala amayinja ge ag’omuwendo.
1161:11 Zab 85:11Kuba nga ettaka bwe livaamu ebimera,
era ng’ennimiro bwereetera ensigo okumeruka,
bw’atyo Mukama Katonda bwalireeta obutuukirivu n’ettendo okumeruka,
ensi zonna zikirabe.