Nyimbo za Mayamiko
1Tsiku limenelo aliyense wa inu adzati:
“Ndikukuyamikani, Inu Yehova;
chifukwa ngakhale munandipsera mtima,
mkwiyo wanu wachoka,
ndipo mwanditonthoza.
2Zoonadi, Mulungu ndiye Mpulumutsi wanga;
ndidzamudalira ndipo sindidzachita mantha.
Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga;
Iye wakhala chipulumutso changa.”
3Mudzakondwera popeza Yehova
ali ngati chitsime cha chipulumutso chanu.
4Tsiku limenelo mudzati:
“Yamikani Yehova, tamandani dzina lake;
mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu,
ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.
5Imbirani Yehova, pakuti wachita ntchito zazikulu;
zimenezi zidziwike pa dziko lonse lapansi.
6Fuwulani ndi kuyimba mwachimwemwe, inu anthu a ku Ziyoni;
pakuti Woyerayo wa Israeli ndi wamkulu pakati panu.”
Songs of Praise
1In that day you will say:
“I will praise you, Lord.
Although you were angry with me,
your anger has turned away
and you have comforted me.
2Surely God is my salvation;
I will trust and not be afraid.
The Lord, the Lord himself, is my strength and my defense12:2 Or song;
he has become my salvation.”
3With joy you will draw water
from the wells of salvation.
4In that day you will say:
“Give praise to the Lord, proclaim his name;
make known among the nations what he has done,
and proclaim that his name is exalted.
5Sing to the Lord, for he has done glorious things;
let this be known to all the world.
6Shout aloud and sing for joy, people of Zion,
for great is the Holy One of Israel among you.”