Salimo 98
Salimo.
1Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,
pakuti Iyeyo wachita zinthu zodabwitsa;
dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera
zamuchitira chipulumutso.
2Yehova waonetsa chipulumutso chake
ndipo waulula chilungamo chake kwa anthu a mitundu ina.
3Iye wakumbukira chikondi chake
ndi kukhulupirika kwake pa Aisraeli;
malekezero onse a dziko lapansi aona
chipulumutso cha Mulungu wathu.
4Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi,
muyimbireni nyimbo mofuwula ndi mokondwera.
5Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze,
ndi zeze ndi mawu a kuyimba,
6ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna
fuwulani mwachimwemwe pamaso pa Yehova Mfumu.
7Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo,
dziko lonse ndi onse amene amakhala mʼmenemo.
8Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo,
mapiri ayimbe pamodzi mwachimwemwe;
9izo ziyimbe pamaso pa Yehova,
pakuti Iye akubwera kudzaweruza dziko lapansi.
Adzaweruza dziko lonse mwachilungamo,
ndi mitundu ya anthu mosakondera.
Песнь 98
1Вечный царствует;
пусть трепещут народы!
Он восседает на херувимах;
пусть содрогнётся земля!
2Вечный велик на Сионе;
Он превознесён над всеми народами.
3Да восхвалят они Твоё великое и грозное имя:
Ты свят!
4Царь могуществен и любит справедливость.
Ты установил правосудие
и в Исраиле98:4 Букв.: «в Якубе». Исраильтяне были потомками Якуба, которому Всевышний дал новое имя – Исраил (см. Нач. 32:27-28). совершил то, что справедливо и праведно.
5Превозносите Вечного, нашего Бога,
и поклонитесь Ему у подножия98:5 Подножие – так обычно называли сундук соглашения, над которым восседал Вечный (см. 1 Лет. 28:2). для ног Его: Он свят!
6Муса и Харун – среди Его священнослужителей,
и Шемуил – среди призывающих имя Его.
Они призывали Вечного,
и Он ответил им.
7В облачном столпе говорил Он к ним;
они сохранили Его заповеди
и установления, которые Он им дал.
8Ты ответил им, о Вечный, наш Бог;
Ты был для них Богом прощающим,
но и наказывал их за проступки.
9Превозносите Вечного, нашего Бога
и прославляйте Его на святой горе Его,
потому что свят Вечный, наш Бог.