Salimo 87
Salimo la Ana a Kora.
1Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2Yehova amakonda zipata za Ziyoni
kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3Za ulemerero wako zimakambidwa,
Iwe mzinda wa Mulungu:
Sela
4“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni
pakati pa iwo amene amandidziwa.
Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi,
ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’ ”
5Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti,
“Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye,
ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina:
“Uyu anabadwira mʼZiyoni.”
Sela
7Oyimba ndi ovina omwe adzati,
“Akasupe anga onse ali mwa iwe.”
Salmo 87
Salmo de los hijos de Coré. Cántico.
1Los cimientos de la ciudad de Dios87:1 Los … de Dios. Lit. Los cimientos de él. están en el santo monte.
2El Señor ama las entradas de Sión
más que a todas las moradas de Jacob.
3De ti, ciudad de Dios,
se dicen cosas gloriosas: Selah
4«Entre los que me reconocen
puedo contar a Rahab y a Babilonia,
a Filistea y a Tiro, lo mismo que a Cus.
Se dice: “Este nació en Sión”».
5De Sión se dirá, en efecto:
«Este y aquel nacieron en ella.
El Altísimo mismo la ha establecido».
6El Señor anotará en el registro de los pueblos:
«Este nació en Sión». Selah
7Y mientras cantan y bailan, dicen:
«Todas mis fuentes están en ti».87:7 Todas mis fuentes. Alt. Todos mis orígenes.