Salimo 87
Salimo la Ana a Kora.
1Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2Yehova amakonda zipata za Ziyoni
kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3Za ulemerero wako zimakambidwa,
Iwe mzinda wa Mulungu:
Sela
4“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni
pakati pa iwo amene amandidziwa.
Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi,
ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’ ”
5Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti,
“Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye,
ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina:
“Uyu anabadwira mʼZiyoni.”
Sela
7Oyimba ndi ovina omwe adzati,
“Akasupe anga onse ali mwa iwe.”
Jerusalem—Guds by og hans folks hjem
1En sang af Koras slægt.
Han grundlagde sin by på de hellige høje.
2Ja, Herren elsker Zions stad
langt mere end andre byer i Israel.
3Jerusalem, du er Guds egen by,
der siges mange herlige ting om dig.
4I Egypten og Babylonien,
i filistrenes land, i Tyrus og Kush
er der folk, der kender Gud
og føler, at Jerusalem er deres hjem.
5I Jerusalem siger man til hinanden:
„Vi hører alle til på dette sted,
og den Almægtige tager hånd om sin by.”
6Herren fører regnskab over alle mennesker,
og noterer dem, der hører Jerusalem til.
7De danser af glæde, mens de lovpriser byen:
„Du er alt, hvad vi har brug for.”