Masalimo 75 – CCL & HOF

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 75:1-10

Salimo 75

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, potsata mayimbidwe a “Musawononge.” Salimo la Asafu. Nyimbo.

1Tikuthokoza Inu Mulungu,

tikuthokoza, pakuti dzina lanu lili pafupi nafe,

anthutu amafotokoza za ntchito zanu zodabwitsa.

2Mumati, “Ine ndimayika nthawi yoyenera,

ndine amene ndimaweruza mwachilungamo.

3Pamene dziko lapansi ndi anthu ake onse anjenjemera,

ndine amene ndimagwiriziza mizati yake molimba.

Sela

4Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’

ndipo kwa oyipa, ‘Musatukulenso nyanga zanu.

5Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba;

musayankhule ndi khosi losololoka.’ ”

6Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo

kapena ku chipululu.

7Koma ndi Mulungu amene amaweruza:

Iyeyo amatsitsa wina, nakwezanso wina.

8Mʼdzanja la Yehova muli chikho

chodzaza ndi vinyo wochita thovu, wosakanizidwa ndi zokometsera;

Iye amamutsanulira pansi ndipo onse oyipa a dziko lapansi

amamwa ndi senga zake zonse.

9Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya;

ndidzayimba matamando kwa Mulungu wa Yakobo.

10Ndidzadula nyanga za onse oyipa

koma nyanga za olungama zidzakwezedwa.

Hoffnung für Alle

Psalm 75:1-11

Schluss mit euren großen Worten!

1Ein Lied von Asaf, nach der Melodie: »Richte nicht zugrunde«.

2Wir danken dir, o Gott – ja, dir allein gilt unser Dank!

Denn du bist uns nahe! Von deinen Wundern erzählen wir.

3Gott spricht: »Wenn meine Zeit gekommen ist,

werde ich Gericht halten und für Gerechtigkeit sorgen!

4Mag auch die Erde beben, und mögen ihre Bewohner vor Angst zittern –

ich selbst habe die Fundamente der Erde unverrückbar festgelegt.

5So befehle ich nun den großmäuligen Angebern:

Schluss mit euren großen Worten!

Denen, die mich ablehnen, sage ich: Blast euch nicht so auf!

6Ja, hört auf zu prahlen und lasst ab von eurem Stolz!75,6 Verse 5b–6a wörtlich: Denen, die mich ablehnen, sage ich: Erhebt nicht das Horn! Erhebt nicht zur Höhe euer Horn!

Tragt eure Nase nicht so hoch!

7Wahre Größe kann kein Mensch verleihen –

ganz gleich, woher er kommt!75,7 Wörtlich: Denn weder vom Osten noch vom Westen noch von der Wüste (= vom Süden) kommt Erhöhung.«

8Denn Gott allein ist Richter:

Den einen lässt er fallen, den anderen bringt er zu Ansehen und Macht.

9Der Herr hat einen Becher in seiner Hand,

gefüllt mit starkem, betäubendem Trank.

Alle, die Gott verachten,

müssen den Becher bis zum letzten bitteren Tropfen austrinken.

10Ich aber will immer von Gott erzählen,

für ihn, den Gott Jakobs, will ich musizieren.

11Er spricht: »Ich werde die Macht der Gottlosen brechen;

doch alle, die zu mir gehören, bringe ich zu Ansehen und Macht75,11 Wörtlich: die Hörner der Treuen werden erhöht werden.