Masalimo 70 – CCL & OL

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 70:1-5

Salimo 70

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho.

1Fulumirani Mulungu kundipulumutsa;

Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.

2Iwo amene akufunafuna moyo wanga

achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa;

onse amene akukhumba chiwonongeko changa

abwezedwe mopanda ulemu.

3Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,”

abwerere chifukwa cha manyazi awo.

4Koma onse amene akufunafuna Inu

akondwere ndi kusangalala mwa Inu;

iwo amene amakonda chipulumutso chanu

nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”

5Koma ine ndine wosauka ndi wosowa;

bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu.

Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga;

Inu Yehova musachedwe.

O Livro

Salmos 70:1-5

Salmo 70

(Sl 40.13-17)

Salmo de David, em memorial. Para o diretor do coro.

1Apressa-te, ó Deus, em me livrar!

Vem depressa em meu auxílio!

2Desmascara e envergonha toda essa gente

que procura matar-me,

esses que querem o meu mal.

3Que sejam obrigados a voltar para trás, a fugir,

esses que pretendem divertir-se à minha custa!

4Mas que se encham de alegria os que te procuram,

os que amam a tua salvação,

e que possam dizer sempre:

“Grande é o poder de Deus!”

5Eu estou aflito e necessitado;

corre em meu auxílio, ó Deus!

Só tu podes ajudar-me e libertar-me;

Senhor, não me faças esperar!