Masalimo 70 – CCL & HTB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 70:1-5

Salimo 70

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho.

1Fulumirani Mulungu kundipulumutsa;

Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.

2Iwo amene akufunafuna moyo wanga

achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa;

onse amene akukhumba chiwonongeko changa

abwezedwe mopanda ulemu.

3Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,”

abwerere chifukwa cha manyazi awo.

4Koma onse amene akufunafuna Inu

akondwere ndi kusangalala mwa Inu;

iwo amene amakonda chipulumutso chanu

nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”

5Koma ine ndine wosauka ndi wosowa;

bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu.

Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga;

Inu Yehova musachedwe.

Het Boek

Psalmen 70:1-6

1Een lied van David voor de koordirigent. Bij het gedenkoffer.

2O God, kom mij snel bevrijden!

Help mij toch, Here!

3Laat de mensen die mij willen ombrengen,

beschaamd staan,

laten zij die mij in het ongeluk willen storten,

terugdeinzen en beschaamd staan.

4Laten zij die mij uitlachen,

maar weglopen van schaamte.

5Laat allen die U zoeken,

juichen en jubelen, zich in U verblijden.

Laten zij die U en uw redding liefhebben,

voortdurend U loven en grootmaken.

6O God, ik zit in grote moeilijkheden

en ben een arm mens.

Kom toch snel naar mij toe.

Alleen U kunt mij helpen en verlossen.

Kom snel, Here,

en wacht niet langer!