Masalimo 67 – CCL & HOF

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.

Hoffnung für Alle

Psalm 67:1-8

Erntedank

1Ein Lied. Mit Instrumenten zu begleiten.

2Gott, sei uns gnädig und segne uns!

Blicke uns freundlich an!

3Dann wird man auf der ganzen Welt erkennen,

wie gut du bist und handelst.

Alle Völker werden sehen und verstehen: Du bist ihre Rettung.

4Die Völker sollen dir danken, Gott!

Ja, alle Völker sollen dich preisen!

5Alle Menschen sollen sich freuen und jubeln,

denn du bist ein gerechter Richter,

du regierst die ganze Welt.

6Die Völker sollen dir danken, Gott!

Ja, alle Völker sollen dich preisen!

7Das Land brachte eine gute Ernte hervor,

unser Gott hat uns reich beschenkt.

8Er segne uns auch weiterhin!

Alle Völker der Erde sollen ihn achten und ehren!