Masalimo 67 – CCL & CCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 67:1-7

Salimo 67

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Salimo.

1Yehova atikomere mtima ndi kutidalitsa,

achititse kuti nkhope yake itiwalire.

2Kuti njira zanu zidziwike pa dziko lapansi,

chipulumutso chanu pakati pa mitundu yonse.

3Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

4Mitundu yonse ya anthu isangalale ndi kuyimba mwachimwemwe,

pakuti inu mumaweruza mitundu ya anthu mwachilungamo

ndi kutsogolera mitundu ya anthu a dziko lapansi.

5Mitundu ya anthu ikutamandeni Inu Mulungu;

mitundu yonse ya anthu ikutamandeni.

6Nthaka yabereka zokolola zake;

tidalitseni Mulungu wathu.

7Mulungu atidalitse

kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.

Chinese Contemporary Bible (Simplified)

诗篇 67:1-7

第 67 篇

赞美上帝

一首诗歌,交给乐长,用弦乐器。

1上帝啊,求你恩待我们,

赐福给我们,笑颜垂顾我们。(细拉)

2这样,普世都会知道你的道路,

万国都会知道你的拯救之恩。

3上帝啊,

愿列邦都赞美你,

愿万族都称颂你。

4愿列国欢呼歌唱,

因为你以公义审判列邦,

引导世上的列国。(细拉)

5上帝啊,愿列邦赞美你,

愿万族都称颂你。

6大地出产丰富。

上帝,我们的上帝要赐福我们。

7上帝要赐福我们,

普天下都要敬畏祂。