Masalimo 54 – CCL & HOF

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 54:1-7

Salimo 54

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Pa zoyimbira za zingwe. Ndakatulo ya Davide. Pamene anthu a ku Zifi anapita kwa Sauli ndipo anati, “Kodi Davide sakubisala pakati pathu.”

1Pulumutseni Inu Mulungu, mwa dzina lanu;

onetsani kuti ndine wosalakwa mwamphamvu yanu.

2Imvani pemphero langa, Inu Mulungu

mvetserani mawu a pakamwa panga.

3Alendo akundithira nkhondo;

anthu ankhanza akufunafuna moyo wanga,

anthu amene salabadira za Mulungu.

4Zoonadi Mulungu ndi thandizo langa;

Ambuye ndiye amene amandichirikiza ine.

5Lolani kuti choyipa chifike pa iwo amene amandichita chipongwe;

mwa kukhulupirika kwanu awonongeni.

6Ine ndidzapereka nsembe yaufulu kwa Inu;

ndidzatamanda dzina lanu, Inu Yehova,

pakuti ndi labwino.

7Pakuti Iyeyo wandipulumutsa ku masautso anga onse,

ndipo maso anga apenya kupambana kwa pa adani anga.

Hoffnung für Alle

Psalm 54:1-9

Nur du kannst helfen!

1Von David, zum Nachdenken. Mit Saiteninstrumenten zu begleiten.

2Dieses Lied stammt aus der Zeit, als die Sifiter zu Saul gekommen waren, um ihm mitzuteilen: »David hält sich bei uns versteckt!«54,2 Vgl. 1. Samuel 23,19; 26,1.

3Gott, mach deinem Namen Ehre und hilf mir!

Verschaffe mir Recht durch deine Kraft!

4Gott, höre mein Gebet,

achte auf mein Schreien!

5Menschen, die ich nicht kenne, fallen über mich her.

Sie schrecken vor keiner Gewalttat zurück,

ja, sie trachten mir nach dem Leben.

Du, Gott, bist ihnen völlig gleichgültig!

6Aber ich weiß: Gott ist mein Helfer,

der Herr setzt sich stets für mich ein.

7Er wird dafür sorgen, dass meine Feinde

durch ihre eigene Bosheit zu Fall kommen.

Ja, Gott, beseitige sie! Du bist doch treu!

8Mit frohem Herzen will ich dir Opfer bringen,

ich will dich preisen, Herr, denn du bist gut.

9Aus jeder Not hast du mich errettet,

nur so konnte ich die Feinde besiegen.