Salimo 53
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Potsata mayimbidwe a Mahalati. Ndakatulo ya Davide.
1Chitsiru chimati mu mtima mwake,
“Kulibe Mulungu.”
Iwo ndi oyipa ndipo njira zawo ndi zonyansa;
palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino.
2Mulungu kumwamba amayangʼana pansi pano
pa ana a anthu
kuti aone ngati alipo wina wanzeru,
wofunafuna Mulungu.
3Aliyense wabwerera,
iwo onse pamodzi akhala oyipa;
palibe ndi mmodzi yemwe amene amachita chabwino,
ngakhale mmodzi.
4Kodi anthu ochita zoyipawa adzaphunziradi;
anthu amene amadya anthu anga monga mmene anthu amadyera buledi,
ndipo sapemphera kwa Mulungu?
5Iwo anali pamenepo atathedwa nzeru ndi mantha aakulu
pamene panalibe kanthu kochititsa mantha.
Mulungu anamwazamwaza mafupa a anthu amene anakuthirani nkhondo;
inuyo munawachititsa manyazi, pakuti Mulungu anawanyoza.
6Ndithu, chipulumutso cha Israeli nʼchochokera ku Ziyoni!
Pamene Mulungu adzabwezeretsanso ulemerero wa anthu ake,
lolani Yakobo akondwere ndi Israeli asangalale!
สดุดี 53
(สดด.14:1-7)
(ถึงหัวหน้านักร้อง ตามทำนองมาหะลัท มัสคิล53:0 หัวเรื่องสดุดี 53 คงจะเป็นศัพท์ทางวรรณกรรมหรือทางดนตรีของดาวิด)
1คนโง่รำพึงอยู่ในใจว่า
“ไม่มีพระเจ้า”
พวกเขาเสื่อมทรามและวิถีทางของพวกเขาก็ชั่วช้าสามานย์
ไม่มีสักคนที่ทำดี
2พระเจ้าทอดพระเนตรลงมาจากฟ้าสวรรค์
ดูมวลมนุษยชาติ
เพื่อดูว่ามีสักคนไหมที่เข้าใจ
มีสักคนไหมที่แสวงหาพระเจ้า
3ทุกคนได้หันหนีไปหมด
พวกเขากลายเป็นคนเสื่อมทรามไปด้วยกัน
ไม่มีสักคนที่ทำดี
ไม่มีแม้แต่คนเดียว
4พวกคนชั่วไม่รับรู้อะไรเลยหรือ?
พวกเขากลืนกินประชากรของเราดั่งอาหาร
พวกเขาไม่เคยร้องทูลพระเจ้า
5ดูสิ พวกเขาจมอยู่ในความตาย
ที่ซึ่งไม่มีอะไรน่าหวาดหวั่น
พระเจ้าทรงทำให้กระดูกของบรรดาผู้ที่โจมตีเจ้ากระจัดกระจาย
เจ้าจะทำให้พวกเขาอับอายขายหน้า เพราะพระเจ้าทรงรังเกียจพวกเขา
6ขอให้การช่วยกู้เพื่ออิสราเอลมาจากศิโยนเถิด!
เมื่อพระเจ้าทรงทำให้เหล่าประชากรของพระองค์กลับสู่สภาพดีดังเดิม
ให้ยาโคบชื่นชมยินดีและอิสราเอลเปรมปรีดิ์เถิด!