Masalimo 42 – CCL & BDS

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 42:1-11

BUKU LACHIWIRI

Masalimo 42–72

Salimo 42

Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya ana a Kora.

1Monga mbawala ipuma wefuwefu kufunafuna mitsinje yamadzi,

kotero moyo wanga upuma wefuwefu kufunafuna Inu Mulungu.

2Moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Mulungu, lofuna Mulungu wamoyo.

Kodi ndipite liti kukakumana ndi Mulungu?

3Misozi yanga yakhala chakudya changa

usana ndi usiku,

pamene anthu akunena kwa ine tsiku lonse kuti,

“Mulungu wako ali kuti?”

4Zinthu izi ndimazikumbukira

pamene ndikukhuthula moyo wanga:

momwe ndinkapitira ndi gulu lalikulu,

kutsogolera mayendedwe a ku Nyumba ya Mulungu

ndi mfuwu yachimwemwe ndi mayamiko

pakati pa anthu a pa chikondwerero.

5Nʼchifukwa chiyani uli ndi chisoni, iwe moyo wanga?

Nʼchifukwa chiyani wakhumudwa iwe mʼkati mwanga?

Yembekezera Mulungu,

pakuti ndidzamulambirabe,

Mpulumutsi wanga ndi 6Mulungu wanga.

Moyo wanga uli ndi chisoni mʼkati mwanga

kotero ndidzakumbukira Inu

kuchokera ku dziko la Yorodani,

ku mitunda ya Herimoni kuchokera ku phiri la Mizara.

7Madzi akuya akuyitana madzi akuya

mu mkokomo wa mathithi anu;

mafunde anu onse obwera mwamphamvu

andimiza.

8Koma usana Yehova amalamulira chikondi chake,

nthawi ya usiku nyimbo yake ili nane;

pemphero kwa Mulungu wa moyo wanga.

9Ine ndikuti kwa Mulungu Thanthwe langa,

“Nʼchifukwa chiyani mwandiyiwala?

Nʼchifukwa chiyani ndiyenera kuyenda ndikulira,

woponderezedwa ndi mdani?”

10Mafupa anga ali ndi ululu wakufa nawo

pamene adani anga akundinyoza,

tsiku lonse akunena kuti,

“Mulungu wako ali kuti?”

11Bwanji ukumva chisoni,

iwe mtima wanga?

Chifukwa chiyani ukuvutika chonchi mʼkati mwanga?

Khulupirira Mulungu, pakuti ndidzamutamandanso,

Iye amene ali thandizo langa ndi Mulungu wanga.

La Bible du Semeur

Psaumes 42:1-12

Deuxième livre

Soif de Dieu !

1Au chef de chœur. Méditation42.1 Signification incertaine. des Qoréites42.1 Descendants de Qoré, l’un des fils de Lévi (Ex 6.24 ; Nb 16 ; 26.11). Ils devinrent musiciens dans le tabernacle (1 Ch 6.18, 22) et portiers (1 Ch 26.1). Leur chef, du temps de David, était Hémân (88.1)..

2Comme une biche tourne la tête ╵vers le cours d’eau,

je me tourne vers toi, ô Dieu42.2 Autre traduction : Comme une biche soupire après les cours d’eau, je soupire après toi, ô Dieu. !

3J’ai soif de Dieu, ╵du Dieu vivant !

Quand donc pourrai-je aller ╵et me présenter devant Dieu ?

4Mes larmes sont le pain ╵de mes jours comme de mes nuits.

Sans cesse, on me répète :

« Ton Dieu, où est-il donc ? »

5Alors que j’épanche mon cœur, ╵je me souviens du temps

où, avec le cortège, ╵je m’avançais,

marchant avec la foule ╵vers le temple de Dieu,

au milieu de la joie ╵et des cris de reconnaissance

de tout un peuple en fête.

6Pourquoi donc, ô mon âme, ╵es-tu si abattue

et gémis-tu sur moi ?

Mets ton espoir en Dieu ! ╵je le louerai encore,

car il est mon Sauveur.

7Mon Dieu42.7 Certains rattachent ces mots à la fin du v. 6 et traduisent : car il est mon Sauveur, il est mon Dieu. 7 Je suis…, mon âme est abattue !

Voilà pourquoi, je pense à toi ╵du pays du Jourdain,

des cimes de l’Hermon ╵et du mont Mitséar42.7 L’Hermon constituait la frontière nord du pays de la promesse (Dt 3.8 ; Jos 11.17 ; 13.11 ; 1 Ch 5.23). Le mont Mitséar ou Petit-Mont n’est cité nulle part ailleurs..

8Un abîme en appelle un autre, ╵au grondement de tes cascades ;

tous tes flots et tes lames ╵ont déferlé sur moi.

9Que, le jour, l’Eternel ╵me montre son amour :

je passerai la nuit ╵à chanter ses louanges

et j’adresserai ma prière ╵au Dieu qui me fait vivre.

10Car je veux dire à Dieu, ╵lui qui est mon rocher :

« Pourquoi m’ignores-tu ?

Pourquoi donc me faut-il ╵vivre dans la tristesse,

subissant l’oppression ╵de l’ennemi ? »

11Mes membres sont meurtris, ╵mes ennemis m’insultent,

sans cesse, ils me demandent : ╵« Ton Dieu, où est-il donc ? »

12Pourquoi donc, ô mon âme, ╵es-tu si abattue, ╵et gémis-tu sur moi ?

Mets ton espoir en Dieu ! ╵Je le louerai encore,

mon Sauveur et mon Dieu.