Masalimo 38 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 38:1-22

Salimo 38

Salimo la Davide. Kupempha.

1Yehova musandidzudzule mutapsa mtima

kapena kundilanga muli ndi ukali.

2Pakuti mivi yanu yandilasa,

ndipo dzanja lanu latsika ndipo landifikira.

3Chifukwa cha ukali wanu mulibe thanzi mʼthupi langa;

mafupa anga alibe mphamvu chifukwa cha tchimo langa.

4Kulakwa kwanga kwandipsinja

ngati katundu wolemera kwambiri kuposa mphamvu zanga.

5Mabala anga akuwola ndipo akununkha

chifukwa cha uchitsiru wa moyo wanga wauchimo.

6Ine ndapindika msana ndipo ndawerama kwambiri;

tsiku lonse ndimangolira.

7Msana wanga wagwidwa ndi ululu wosasimbika,

mulibe thanzi mʼthupi langa.

8Ndilibe mphamvu ndipo ndakunthidwa kwathunthu;

ndikubuwula ndi ululu wa mumtima.

9Zokhumba zanga zonse zili poonekera pamaso panu Ambuye,

kusisima kwanga sikunabisike kwa Inu.

10Mtima wanga ukugunda, mphamvu zanga zikutha;

ngakhale kuwala kwachoka mʼmaso mwanga.

11Abwenzi anga ndi anzanga akundipewa chifukwa cha mabala anga;

anansi anga akhala kutali nane.

12Iwo amene akufunafuna moyo wanga atchera misampha yawo,

oti andipwetekewo amayankhula za kuwonongeka kwanga;

tsiku lonse amakonza zachinyengo.

13Ine ndili ngati munthu wosamva amene sangamve,

monga wosayankhula, amene sangathe kutsekula pakamwa pake;

14Ndakhala ngati munthu amene samva,

amene pakamwa pake sipangathe kuyankha.

15Ndikudikira Inu Yehova;

mudzayankha, Inu Ambuye Mulungu wanga.

16Pakuti Ine ndinati, “Musawalole kuti akondwere

kapena kudzikweza okha pa ine pamene phazi langa laterereka.”

17Pakuti ndili pafupi kugwa,

ndipo ndikumva kuwawa nthawi zonse.

18Ndikuvomereza mphulupulu zanga;

ndipo ndavutika ndi tchimo langa.

19Ambiri ndi adani anga amphamvu;

amene amandida popanda chifukwa alipo ochuluka kwambiri.

20Iwo amene amandibwezera zoyipa mʼmalo mwa zabwino

amandinyoza pamene nditsatira zabwino.

21Inu Yehova, musanditaye;

musakhale kutali ndi ine Mulungu wanga.

22Bwerani msanga kudzandithandiza,

Inu Ambuye Mpulumutsi wanga.

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 38:1-22

Zabbuli 38

Zabbuli ya Dawudi, ey’okujjukiza.

138:1 Zab 6:1Ayi Mukama tonnenya ng’okyaliko obusungu,

oba okunkangavvula ng’oliko ekiruyi.

238:2 Yob 6:4; Zab 32:4Kubanga obusaale bwo bunfumise,

n’omuggo gwo gunkubye nnyo.

338:3 Zab 6:2; Is 1:6Obusungu bwo bundwazizza nzenna,

n’amagumba gange gonna gansagala olw’ebyonoono byange.

438:4 Ezr 9:6Omusango gwe nzizizza guyitiridde,

gunzitoowerera ng’omugugu omunene oguteetikkika.

538:5 Zab 69:5Ebiwundu byange bitanye era biwunya,

olw’okwonoona kwange okw’obusirusiru.

638:6 Yob 30:28; Zab 35:14; 42:9Nkootakoota era mpweddemu ensa,

ŋŋenda nsinda obudde okuziba.

738:7 Zab 102:3Omugongo gunnuma nnyo,

ne mu mubiri gwange temukyali bulamu.

838:8 Zab 22:1Sikyalimu maanyi era nzenna mmenyesemenyese;

nsinda buli bbanga olw’obulumi mu mutima.

938:9 Yob 3:24; Zab 6:6; 10:17Mukama, bye neetaaga byonna obimanyi,

n’okusinda kwange okuwulira.

1038:10 a Zab 31:10 b Zab 6:7Omutima gumpejjawejja, amaanyi gampweddemu;

n’okulaba sikyalaba.

1138:11 Zab 31:11Mikwano gyange ne be nayitanga nabo banneewala olw’amabwa gange;

ne bannange tebakyansemberera.

1238:12 a Zab 140:5 b Zab 35:4; 54:3 c Zab 35:20Abaagala okunzita bantega emitego,

n’abo abangigganya bateesa okummalawo.

Buli bbanga baba bateesa kunkola kabi.

13Ndi ng’omuggavu w’amatu, atawulira;

nga kiggala, atayogera.

14Nfuuse ng’omuntu atalina ky’awulira,

atasobola kwanukula.

1538:15 a Zab 39:7 b Zab 17:6Ddala ddala nnindirira ggwe, Ayi Mukama,

onnyanukule, Ayi Mukama Katonda wange.

1638:16 a Zab 35:26 b Zab 13:4Tobakkiriza kunneeyagalirako,

oba okunneegulumirizaako ng’ekigere kyange kiseeredde.

17Kubanga nsemberedde okugwa,

era nga nnumwa buli kiseera.

1838:18 Zab 32:5Ddala ddala njatula ebyonoono byange;

nnumirizibwa ekibi kyange.

1938:19 a Zab 18:17 b Zab 35:19Abalabe bange bangi era ba maanyi;

n’abo abankyayira obwereere bangi nnyo.

2038:20 Zab 35:12; 1Yk 3:12Abalabe bange bankyawa olw’okuba omulongoofu,

era bwe nkola ebirungi banjogerako ebitasaana.

2138:21 Zab 35:22Ayi Mukama, tonjabulira;

tobeera wala nange, Ayi Katonda wange.

2238:22 a Zab 40:13 b Zab 27:1Ayi Mukama Omulokozi wange,

yanguwa okumbeera.