Masalimo 30 – CCL & KLB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 30:1-12

Salimo 30

Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba popereka Nyumba ya Mulungu.

1Ndidzakukwezani Yehova,

chifukwa mwanditulutsa kwakuya,

ndipo simunalole kuti adani anga akondwere pa ine.

2Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo

ndipo Inu munandichiritsa.

3Inu Yehova, munanditulutsa ku manda,

munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje.

4Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika;

tamandani dzina lake loyera.

5Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi

koma kukoma mtima kwake ndi kwa moyo wonse;

utha kuchezera kulira usiku wonse,

koma chimwemwe chimabwera mmawa.

6Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati,

“Sindidzagwedezekanso.”

7Inu Yehova, pamene munandikomera mtima,

munachititsa phiri langa kuyima chilili;

koma pamene munabisa nkhope yanu,

ndinataya mtima.

8Kwa Inu Yehova ndinayitana;

kwa Ambuye ndinapempha chifundo;

9“Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga

ngati nditsikira ku dzenje?

Kodi fumbi lidzakutamandani Inu?

Kodi lidzalengeza za kukhulupirika kwanu?

10Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo;

Yehova mukhale thandizo langa.”

11Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina;

munachotsa chiguduli changa ndi kundiveka ndi chimwemwe,

12kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete.

Yehova Mulungu wanga, ndidzapereka kwa Inu mayamiko kwamuyaya.

Korean Living Bible

시편 30:1-12

감사의 기도

(다윗의 시. 성전 봉헌식 때 부른 노래)

1여호와여,

내가 주를 찬양합니다.

주께서는 나를

내 대적에게서 구하시고

그들이 나에게

으스대지 못하게 하셨습니다.

2여호와 나의 하나님이시여,

내가 주께 부르짖었더니

주께서 나를 고쳐 주셨습니다.

3여호와여, 주께서는

30:3 또는 ‘내 영혼을 음부에서 끌어내어’나를 죽음 직전에서 구출하시고

나를 무덤으로

들어가지 않게 하셨습니다.

4여호와의 성도들아,

주께 노래하고

그 거룩한 이름을 찬양하여라.

5그의 노여움은 잠깐이요

그의 은총은 평생 동안이다!

밤에는 우는 일이 있을지라도

아침에는 기쁨이 오리라.

6내가 30:6 또는 ‘형통할 때’안전할 때에

“나는 결코 흔들리지 않으리라”

하였습니다.

7여호와여, 주께서 나에게

은혜를 베풀었을 때에는

나를 산처럼 굳게 세우셨는데

주의 얼굴을 가리셨을 때에는

내가 두려워하였습니다.

8여호와여, 내가 주께 부르짖고

이렇게 간구하였습니다.

9“내가 무덤에 내려가면

주께 무슨 유익이 있습니까?

30:9 또는 ‘진토가’죽은 자들이

주를 찬양할 수 있겠습니까?

그들이 주의 성실하심을

선포할 수 있겠습니까?

10여호와여, 들으시고

나를 불쌍히 여기소서.

여호와여, 나를 도와주소서.”

11그때 주께서는

나의 슬픔이 변하여

30:11 또는 ‘춤이’기쁨이 되게 하셨으며

내게서 슬픔의 옷을 벗겨 주시고

기쁨의 띠를 띠워 주셨습니다.

12그래서 내가 침묵을 지키지 않고

주께 찬양합니다.

여호와 나의 하나님이시여,

내가 주께 영원히 감사하겠습니다.