Masalimo 24 – CCL & LCB

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Masalimo 24:1-10

Salimo 24

Salimo la Davide.

1Dziko lapansi ndi la Yehova ndi zonse zimene zili mʼmenemo,

dziko ndi onse amene amakhala mʼmenemo;

2pakuti Iye ndiye anayika maziko ake pa nyanja

ndi kulikhazika pamwamba pa madzi.

3Ndani angakwere phiri la Yehova?

Ndani angathe kuyima pa malo ake opatulika?

4Iye amene ali ndi mʼmanja moyera ndi mtima woyera,

amene sapereka moyo wake kwa fano

kapena kulumbira mwachinyengo.

5Iyeyo adzalandira madalitso kwa Yehova

ndipo Mulungu mpulumutsi wake adzagamula kuti alibe mlandu.

6Umenewo ndiwo mʼbado wa amene amafunafuna Yehova;

amene amafunafuna nkhope yanu, Inu Mulungu wa Yakobo.

Sela

7Tukulani mitu yanu inu zipata;

tsekukani, inu zitseko zakalekalenu,

kuti Mfumu yaulemerero ilowe.

8Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?

Yehova Wamphamvuzonse,

Yehova ndiye wamphamvu pa nkhondo.

9Tukulani mitu yanu, inu zipata;

tsekukani, inu zitseko zakalekalenu,

kuti Mfumu yaulemerero ilowe.

10Kodi Mfumu yaulemereroyo ndani?

Yehova Wamphamvuzonse,

Iye ndiye Mfumu yaulemerero.

Sela

Luganda Contemporary Bible

Zabbuli 24:1-10

Zabbuli 24

Zabbuli ya Dawudi.

124:1 a Kuv 9:29; Yob 41:11; Zab 89:11 b 1Ko 10:26*Ensi ya Mukama n’ebigirimu byonna,

n’ensi zonna n’abo abazibeeramu.

2Kubanga yasimba emisingi gyayo mu nnyanja,

n’agizimba ku mazzi amangi.

324:3 a Zab 2:6 b Zab 15:1; 65:4Alyambuka ku lusozi lwa Mukama ye afaanana atya?

Era wa ngeri ki aliyingira n’ayimirira mu nnyumba ye entukuvu?

424:4 a Yob 17:9 b Mat 5:8Oyo alina omutima omulongoofu, nga n’emikono gye mirongoofu;

atasinza bakatonda abalala,

era atalayirira bwereere.

5Oyo Mukama anaamuwanga omukisa,

n’obutuukirivu okuva eri Katonda ow’obulokozi bwe.

624:6 Zab 27:8Ogwo gwe mulembe gw’abo abakunoonya,

Ayi Katonda wa Yakobo.

724:7 a Is 26:2 b Zab 97:6; 1Ko 2:8Mweggulewo, mmwe bawankaaki!

Muggulwewo, mmwe enzigi ez’edda,

Kabaka ow’ekitiibwa ayingire.

824:8 Zab 76:3-6Kabaka ow’ekitiibwa ye ani?

Ye Mukama ow’amaanyi era ow’obuyinza,

omuwanguzi mu ntalo.

9Mweggulewo, mmwe bawankaaki,

muggulwewo mmwe enzigi ez’edda!

Kabaka ow’ekitiibwa ayingire.

10Kabaka ow’ekitiibwa oyo ye ani?

Mukama Ayinzabyonna;

oyo ye Kabaka ow’ekitiibwa.